Email a copy of 'First Lady urges Comesa to invest in girl child education: To create an empowered generation of women' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

7 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
alukosyo
alukosyo
9 years ago

koma decoration ya nkhope ngati choumba mwa yenjeza mukufuna kuoneka ngati chani. ma ring mmanja dzasatanic!

Wiltone mataka
Wiltone mataka
9 years ago

Alwayz galz nt boyz! Koma lizakhalako bungwe loona abambo nd anyamata?

Kwasakwasa
Kwasakwasa
9 years ago

Kaudzudzu akanso inu!! Kodi ndi udzudzu wanji uwu wotchedwa Getrude Maseko Mutharika?

Van Persey
Van Persey
9 years ago

I am always surprised why African leaders take their wives to summits. Look now that it is becoming a trend to organize parallel so called First Lady summits which are practically useless. These useless parallel summits are an extra financial burden on host Governments

Bwitoto
Bwitoto
9 years ago

Girl childyo mwamudziwa muli ku Sanjika? Tamusiileni JB zimenezo inu simungazithe. Tangopitilizani zaulaiya ndi kukokola zinyalala mmadzalamu. Bola musabenso ku bungwe lina.Paja inu kukonda kuba ndi makani opanda nzeru. Mxiiiiew!!!!!!!

dumie gondwe
dumie gondwe
9 years ago

wat abt a boy child, unangokula ulibe nzeru

Nam'bwibwi
9 years ago

Awanso ndie amandinyansa bwanji,analowa m’gulu la anthu akuba,amunawo akutinamiza kuti ali ndi over K840 million koma kulephela kupanga ukwati kuchita kudalila anthu akufuna kwabwino,kulephela kupeleka ndalama ku mulakho,ndi BEAM mkuba ndalama ku NAC ndipo mapeto ake NAC ili m’madzi,kutinamiza kuti anakana salary increament koma pomwe amazidziwa mpakana Nankhumwa kulengeza,kutinamiza kuti Bingu adakali ndi moyo pomwe atamwalila,kuti namiza anthu kuti ndi Daniel Phiri, kutinamiza kuti vitara value yake ndi k51 m,ndi zambiri ndipo ndikuuzanibe,komano chomwe ndachiona nchakuti APM alibe chili chonse,mano alibe(mwina pano anagula) chisoni alibe,luso loyankhula alibe,mapulani otukula malawi alibe,ulemu alibe,nzelu alibenso.

Read previous post:
Researching the politics of public sector reforms in Malawi

The Effective States and Inclusive Development (ESID) Research Programme has commissioned a multi-country study on the comparative politics of public sector reforms (PSR)...

Close