Email a copy of 'Husband hacked to death by ‘jealous’ wife in Malawi gruesome murder' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Husband hacked to death by ‘jealous’ wife in Malawi gruesome murder' to a friend
After a season of so much torment and frustration, and facing the prospect of a relagation, Mighty Wanderers seem to...
Amayi Kaliya muli kuti? A Seodi White muli kuti? Nanga a Jesse Kabwila muli kuti? Uyunso ndinaiwala Kwataine Marita mulipo? We hear make more comments when men have done something bad on women why don’t you condemn this unbecoming behaviour by this young lady kupha mwamuna ngati apha nkhumba kapena ng’ombe? If it were mkazi waphedwa in such a brutal manner media yonse kunali gwedegwede kodi ziditero? Gender equality mumaifunayo ndi iti? One thing you shud know sizidzatheka kukhala gender equality ayi. Mwamuna sadzatengapo mimba wosatheka mkazi sizidzatheka kupereka mimba kwa mkazi ayi. So zinazi ndi bwino kuazimasulira bwino otherwise… Read more »
women r bad
Zomvesa chisoni amuna onsewa mwina ndi mufti
Tiko, Number 64, the couple was from Ntchisi and went to Nkhata Bay for ntchito ya ”utenant.”
The lady is only 21 against this man 32. Is this not childish kind of behaviour. Atonga a Bura ndiye yapa chavuta uri?
SAMVA ZANZAKE ANAMVA NKHWANGWA ILI MMUTU…..KOMA APA MATHU MWAONJEZA. MUKANANGOSAMUKA NGATI SAMAMVA MWAMUNAYO NDIKUKAKHALA KWANU KWABWINOKO. MUKANAFUNSA MMENE MKAZI NZANU WA “”MESHO” ( WIFE TO KAMOWA) ANACHITILA.ANANGOSAMUKA AND FILED FOR DIVORCE…I CONGRATULATE HER HER AND WISH ALL PRESSED IN THEIR MARRIEGES SHOULD EMULATE SUCH A COMMENDABLE ACTION OSATI MAZUNZO A NDENDE MWAPUTA APAWA!!!!!!!!!
Ayi,akanayenela kubwenzerapo chilango cha malemu kamuzu banda chija,wopha mzake nayeso aphedwe.mwina anthu angaphunzire kukhululukilana.zomvesa chisoni kwambiri.
Mulungu atithandize.kumeneko timati kusowa mzimu.mwana wa mwini kumulimbira mtima choncho?Bwanji osangomuleka nawe kutengana ndi amuna ena?satana wakuchenjererani mai.
Simunati………… mukhalapana
womens groups please comment