Email a copy of 'Kabwila faces arrest for ‘treason’ over Whatsapp discussion: Malawi opposition aide accused of inciting 'regime change'' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Kabwila faces arrest for ‘treason’ over Whatsapp discussion: Malawi opposition aide accused of inciting 'regime change'' to a friend
Football Association of Malawi (FAM) president Walter Nyamilandu says the era of having unqualified coaches in the game of football is...
Kabwira nanga bwanji amachita makani ngati ali ndi machende pomwe kwake nkomyatara. Ngati ali kafa nikhale osakhala poonekera bwanji kuti a munjate- akuthawiranji? – khwangala wa mkazi. zimachita kudziwikiratu kuti phokoso lomwe amachita lija nilosonyeza kuti ali pa heat, ndiyeno zikati zisayende, mafrastraions kumangobwebwetano. A mmange basi adziwe kuti boma ndi chanji – she is abusing her freedom of expression. How can you plan topple the government knowing very well we shall have elections in 2019, why not wait and plan you campaign when time comes? While I agree with those people who have faulted government for going too far… Read more »
Chigumula mukuoneka kuti ndinu.munthu oziwa malembo komano what u can add on ur comment is we are in.the lastdays this things have to happen. Dont point fingures to anybody. kodi bible silinakambe abt the signs of the time drought, wars, kusowa chikondi and so on. so u want this things to happen rt? kodi Mulungu anayamba wanamapo? let me tell u this, you cant prevent this stuation u dnt ve any power and no one has. let the prophecy be fullfilled u cant fix this problem . tiyeni tipemphere kwambili Ambuye akonze myoyo yathu that nomatter hw big problems but… Read more »
A couch omwe anatengere timu ku Angola, anachotsedwa atalephera ku builder team. Lero wina awanena maganizo ake, mwati mangani. Ndiye mumnga anthu angati kuti anthu apezechimanga chakudya, apeze mankhwala ku zipatala. Inflation muthane nayo Zamanyazi. Osangovovemera kuti zanivuta wina andilandire kuti tikafike. Mangani enawo muike dziko pamoto. Mukuona ngati kuti amaene tidakuvoterani, ulamulilo wanu tikukondwera nawo Ata! Makolo athu akuvutika chifukwa cha inu Mumangenso ena lero mawanso mumangenso ena mawa. Muone Malawi walero. Mmene ife ti chete muganiza kuti zikutisangalalatsa. Pepani!
Qwq O Kabwira Onjate ophunzire kupereka ulemu kotsogoleri odziko osamayese kuyendetsa dziko kuti nkofanana nkoimbira vilombo va gule wa mkulu monga omakanja, obamba ndo okang’wing’wi
A Peter dzanja lalemba. Tinkanena kuti you can rig and lie to the whole world that you are a God chosen king. It has just been a matter of time. You cant rule because the grace and anointing of God is not on you. God never appointed you. You were a self-imposed leader. God does not bless thieves, liars and cheaters. you guys stole during the Bingu era. Heaven still has those records. You guys killed so many including robert chasowa. You think heaven has forgotten. With your right hand you go to USA to get money to promote sodomy.… Read more »
MUDZILEMBA MA NAMES ENI ENI NDI DZIKUONANI MMALO MOTI MU DZI COMMENT ZA NZERU NTCHITO KUTUKWANA BASI AKUMANGENI ANYAWU INU, WINA WADYA ZA MATHANYULA KWA AMERICA UKO SOME WEEKS AGO MUUZE KUTI NDI UMPAWI WAKEWO AKADZIBWENZA DZIMENEZO MA PLAN AKEWO SATHEKA, ACHITE CHI PUSH BACK NGATI PUMBWA APA.
IN SHORT. TO BE ON THE SAFE SIDE, POFUNIKA KUSIYA COMMENTING OR SPEAKING YR MIND ON SOCIAL MEDIA; IE FACEBOOK, TWEETER, WHATSAPP EVEN NYASATIMES CONCERNING GOVERNMENT OR ANYTHING THAT CAN INVITE TROUBLE IN YR LIFETME. TINGAZUNZITSE MTUNDU WA ANTHU AMENE AMATIDALIRA SINCE WE ARE being monitored on the internet Villagelly, Districally, Nationally, Internationally and perharps globally . I REST HERE AND NOW.
How contradicting! You are not afraid of arrest and at the same time you are hiding? Why? I thought you are running away from arrest??? Anyway, munthu ndichoncho but such obvious contradictions ought to be avoided if people are to take you seriously. Now turning to insinuating the public. You need to be reminded that as long as you are an interested party, people will take your calls with some reservations. Why don’t you let the Civil Society identify the problem (and mobilise for national wide unrest) just as it happened in 2011? Your direct involvement in this is indeed… Read more »
Some weeks ago someone wrote an article about the PAC meeting, its agenda, the involvement of Virginia palmer, chakwera’s funded trip to America and the proposed ouster of the president and my comment was he was it was one of the DPP cadets. Now this reveals it all the very same names mentioned on that article are championing this. Don’t you know Mr chakwera that God time is the best? you were once a man of Yahweh and this philosophy I am sure still remains in your mind, but why? david refused to lay his hand on saul the king… Read more »
What about those who comment on social media such as Nyasatimes? How many will be arrested? Zayambika!