Email a copy of 'Kamlepo says cash-rich ministers boasting with Cashgate money' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Kamlepo says cash-rich ministers boasting with Cashgate money' to a friend
High Court in Blantyre on Tuesday refused an application by Malawi Revenue Authority (MRA) to lift an injunction which was...
ANGULURUCHIRE CHEKAMLEPOWA NI MUNDU WAMIZALA KWAEDYINJI. ZANAVUNE YEKA KUDWALA MIZOTO SINANGOCHITIKA BAASI. NGATI PALI WANDU WACHIVUNDO ADYAULISEDYE KUCHIPATALA CHA MENTO KU SOMBA
AMALAWI a zanga Kamulepo Ndimunthu oti sangagwire mkazi wake akudyedwa Chifukwa ndi waphuma heavy. Akangomva chinthu kuthamanga ku Radio osafufuza kaye, Kamlepo nthawi ya Muluzi Amalimbikira kuti alowa ntchire koma atangopasa ndalama anakhala chete, Chomwe akufuna ndi Ndalama, Kalua Name them you will be heroe but no one can take you serious unless ur fellow northerner
Tough Times Do Not Last But Tough People Do,
Atsongoleri abwino amalakhula pang’ono, ndi kuchita zambiri. Atsongoleri oyipa amalakhula zithu zobveka/ zongopeka koma zopanda umboni. Atsongoleri oyipa sabva bwino wina akakhala pa tsongolo pawo.
Kamlepo, unazolowera ku bera a chair bwana APM sungawabere ndi wamkulu pa za malamulo. Ukuchepera kaba
KAMLEPO IS BETTER THAN PETER AND CHAPONDA……….OUR NORTHERN GIANT
kwali
Do not under estimate Kamlepo! He is the only one who is actullaly telling as it is. Politicians are plundering the economy of this country and nobody is doing absolutely nothing about it. You will remain poor for ever! Kamlepo, carry on doing what is right. Wamisala adaona nkhondo!
Mumamunyoza Kamlepo koma amanena zoona. Dikilani.
SHUT UP Kamplepo you empty tin. Malawi never knew the word cashgate untill PP Reign . stupid