Email a copy of 'Malawi activist protest to S.A Embassy in Lilongwe' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Malawi activist protest to S.A Embassy in Lilongwe' to a friend
Civil society organisations (CSO) have declared that they will not be intimidated by government through Solicitor General Janet Banda that...
y waste time talking about demonstrations which took place last year on 28th april 2014!
Amalawi mwaiwala kuti mulibe zipatala zokafelako ma president anu? Kamuzu ndi Bingu mdapita nao kujoni kuzpatala. Bakiri wachila ndimadotolo aku SA. nanga mulindi ndlama zoti mzapite nao ku Britain akadwala?
Ma players akapita kukaponya mpira kunja ndie kuti ndi pa joloza.
Msalimbane ndijoni. Mangochi, Mzimba pano kulibe nyumba zodinda ndi zaudzu bkoz of johni.
Billy kaunda adaimba kale kuti “Osauka alibe mau” malawi ngosauka. Ali pa position 2 pa whole world
To be fair and square they say Two wrongs dont make a wright. Amalawi msandisekese. Zoona kupanga mademo ati musiya kugula ndugulisa ma products a RSA? Kupenga? chamba? Giving RSA 48 hrs ultimatum? Hehede! Amalawi u cant battle wth RSA. Ziko lathu ndilosaukitsisa. Olemela ndi osauka sangalimbane. Ife amalawi tili in millions kujoni pomwe iwowo muno mwathu alipo less 1000. pafupifupi each home pali zinthu zajoni meaning it is us more benefiting. Akatithamangisa tonse kujoni kodi tizayamba kupita kuti? ku TZ? ZEMBO? MOPUTO? In short we can demostrate koma osawa ophyeza a RSA mwamva? Rsa is halfway our master like… Read more »
Ali pakatiwo mwati ndindani? anyway, good move sasafilika yatiwonjeza–let them pack and Futseki
we can survive without standard bank
Very sad
The Zulu barbaric King and his uncivilised foolish subject must be taught a lesson by boycotting all South African goods. Why on earth butcher fellow African? Do they knnw that if Mandela was butchered in countries where he was seeking refuge then these imbeciles would still under colonialism. These pigs have never been school. Which country on does not unemployment? Which country on earth doesn’t have foreigners? The problem these Vandals have never travelled Outside their province let alone their country as the UK ambassador put it on BBC.
Good Move Guyz
CHITSIRU IWE UZITSIRA NDEMANGA ZENIZENI SIZAMASEWERA IZI AYI
Mwajambulitsatu ngati akaidi akamatengedwa ID for easy identification. Good Ideas though
Lets follow what man of God prophet T.B Joshua said last sunday that Africa shud unite for we cannot correct wrong with another wrong but the right, remember Malawi is a GOD fearing nation.