Email a copy of 'Malawi family in Ireland fights deportation' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Malawi family in Ireland fights deportation' to a friend
A 47-year-old man has died in Chikwawa district after taking medicinal concoction to quit alcohol, police have confirmed. Police, meanwhile,...
ndimaona ngati ndindekha amene sindikumvesa za nkhaniyi,a Nyasatimes times chonde timakupopani tikakhala moyendamu please osamatichitisa manyazi lembani nkhani mwa straight forward osazungulira zungulira
EISH! too bad
Sizikumveka why reporting zinthu zoterezi,pamenezambili mkulephera
Nena how can you let this stupid wife of yours turn you into such an idiot?
Iwe mwana wa bwino zedi wa chilungamo, olimbikira ntchito kukapezeka ndi nkazi ameneyu? Bambo ake akunenawo ngakhaledi anali amatenda ndimayesa anamwalira tinakayika kalekale? Bambo ameneyu wapita atawononga atsikana ambili mu 47. Ana ake onse kuphatikiza nkazi wakoyo anatengela bambo a wo za uhule. Bwerako kumeneko Ana akowo tidzasamala ife abale ako. Usatichititse manyazi ndi Jazebel ameneyu! Osayipitsa dzina LA bambo ako motele!
Lembani nkhani zothandiza Plz.
ka nkazi wayima nako kali bullet.
Your stupidity, zogogulisa ma passport kwa aliyese nde izi, this people are not malawians, anagula ma passport a malawi, kukalowela nawo ku asylum n fake names! I can’t believe how stupid our leaders are, mkhwimitsani malamulo inu, musamangone! Ntchito kumba basi
Mumava bwanji mukamapanga malipoti A boza muzaziona akazakungwilani inuyo ku china mukupita kuja
Peter Nkosi you are stupid….How many people they are living illigaly in UK OR USA.. these people are not the first malawians to apply for assylum …in any country in the world.
why your are not reporting of nigerians ….our president did the same in USA.. SO WHAT?
Malawians open your eyes and see…..our friends are ahead of time …muzipusa choncho
Leave these people alone
Mukutibowa mwamva.