Email a copy of 'Malawi govt pays Mulli K1 billion compensation' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

113 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
ahoy
9 years ago

He supplied nothing n he wants to b paid? Malawi

ahoy
9 years ago

He supplied nothng , y should he be paid? U think Malawians n donors r going to like this? Wait

Thyangathyanga
Thyangathyanga
9 years ago

This is their cash gate now. Its a way of enriching themselves. Am not surprised. Compasation ya 1.3 Billion inachitikako kutiko? Munachotsa ntchito anthu 300 ku MBC, milandu yao mpaka lero mukungowapondereza osawapatsa nao ma compasation awo koma mukukatenga 1.3 billion kumpatsa munthu m’modzi mudzina la compasation. A Malawi siife zitsiru ai, tikuona zimenezi and we will speak at an appropriate time.

Wakumudzi
Wakumudzi
9 years ago

Inentu ndikuwamvetsa anzathu akumpoto. Chuma cha mtundu wa Malawi chitamagawidwa kuzigawo, kukolola kumene kukuchitika kukhoza kutha. Chifykw ndi chakuti, Chigawo chili chonse chizisata kayendesedwe ka chuma chake mowilikiza. Potelo, ndiye kuti chitukuko ku mudzi chingakweleko mwansanga. Ine ndingakondwe kuwona mpikisano wa zigawo pakayendesedwe ka chuma ndi chitukuko.

Ine ndikuwona kuti ambiri amene asakugwilizazan ndi federationyo ndi amene amasolola kapena kupakulu. Tichite manyazi ndithu ife a kwathu kumwela. Tizingokhalira kunyoza ngai kuti sitpemphela? Ayi, tikuwopa chiyani kuti chuma cha Malawi tizigawana ku zigawo, Tikuwopa chiyani?

ankhoma
ankhoma
9 years ago

mmmmm.1billion for compensation am ldreaming? my God this is unfair is apm aware of this? pliz lets stop paying tax.

chosatheka
chosatheka
9 years ago

BWANJI TISIYE KULIPIRA TAX, I MEAN THIS IS NOT FAIR. WE ARE STRUGGLING TO MAKE ENDS MEET AND SOME IDIOT JUST GOES AWAY WITH OUR TAX MONEY. AMALAWI ITS TIME WE STOOD FOR OUR RIGHTS AND FIGHT SO THAT NDALAMA ZATHU ASAMANGOSEWELETSA. AZIBAMBO TIYENI NAZONI – MUSANGOTI DUU NGATI SIMUKUZIONA ZIKUCHITIKAZI!!!!!!!!!!

BigMan
BigMan
9 years ago

If the government owes him money, then why shouldn’t they pay him? Stop barking!

Zikundiopsya
Zikundiopsya
9 years ago

Dzanja la lemba as cashgate continues! Koma 5 year term iyi ………. Tiyeni tione.

comrade
comrade
9 years ago

Zitsiru ndi majudges athu who dont seem to understand remedies for breach of contract in govt contracts!!! It is extremely difficult to show “loss of business profit” on a business transaction that “never happened!”. That is why you never hear such nonsense in transparent and incorruptible economies and countries! I dont know what our “useless judges” use to make it this easy! I can challenge our “useless judges” there is not a single compensation case where the “compensated” can truly show “loss of business profits” for their companies that do not even keep detailed, up-to-date records of business transactions!

Zex
Zex
9 years ago

Then all bids which were lower than the successful bid should be given K1 billion Kwacha by the Malawi Government. Period. It should not be only Mulli.

Read previous post:
Malawi federalism demo ban attacked as ‘censorious’

Malawi human rights groups have condemned government authorities for criminalising peaceful demonstrations, describing the move as worrying, aggressive and censorious....

Close