Email a copy of 'Malawi Police arrest man for stabbing woman over K750 000 debt' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Malawi Police arrest man for stabbing woman over K750 000 debt' to a friend
The First Lady Gertrude Mutharika has called on youths in the country to jealously guard the peace and tranquility that...
kodi zinthuzi ndizakubanja eti? sister wa a guy wa, Sarah, anamuombanso mwamuna wina wake dollar, akuti amakalipira fees yaku Health Science, kenako ndikumathawa guy ikamufunsa.
eeeeeeeish koma anthu ena ake nkhanzaaa……… end time events
Chemjambe, zikuwoneka kutitu mkaziyu ndi yemwe anapereka Dollar kwa man wa. Nde amakumbutsa dollar zache mayiyu pafupipafupi Phiriwa powona kuti dollar yashuzya patauni, anamunamiza mkaziyu kuti akumufuna kuti abweze dollar. Koma anamulakwila kwambiri nanga zache zomwe pilizi???
Okay akulu! Yankhulani mokutha mawa zamanyi zanuzo!
shouldnt he also answer charges of attempted murder?
Ankolo kukongoza ndalama mkazi ndi chimodzimodzi kukataya mu nyanja, mkazi sabwenza ngongole boss. pepani mwaluza kangachepe kanu apa
Its the man who borrowed money from Sally.
Chemjambe, ankolo anuwa ndi omwe anakongola ndalama kwa mkazi osati mkazi kukongola kwa ankolo anuwo. Abaya mkazi chifukwa chokanika kubweza ngongole kwa mkaziyo
Sukulu munadumphira eti………. The man is the one obweleka ndalama ka from the lady…..
Anyway, did he really stabbed her or merely threatened her……. Because there’s no way a multiple stab wound (s) patient can be treated as an outpatient
Abambo man wa ngopusa its him actually who borrowed from the woman ndiye when the woman was asking for her man iwowo basi he decided to silence the woman.
Kodi ndiwaku 18 eti. The power of drinking manyi, amuzunguza ubongo mpaka kubayanzake
That’s bed fear God men