Email a copy of 'Malawi Police fire tear gas at MCP supporters' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Malawi Police fire tear gas at MCP supporters' to a friend
Vice-President Saulos Chilima says it remains government’s mission to move Malawi from aid dependence to trade and become an export-led...
Police
So sad. According to MLS
Chikanakhala Chimanga,tikanakazinga Ndikuchitafuna.Ameneyu Ndiwa satanic,angofuna Tonse Tife Akhale Yekha.Ndichifukwa Chache Nthawi Yovota Ija,njuchi Zimamutsatira,anali Ma Illuminants Amazaponya Nawo Mavoti Kuti Awine.Vampire Opha Anthu Uyu.Mademo Fast,achoke Ameneyu,osamusiya.
Watsala pang’ono uyu Mathanyula. Afa ndi maganizo as zonse zikuchitikazi sangagone nazo tulo ndipo alibe mtendere. Akayesera kugona afera kutulo komweko
Anthu akamati dziko la Malawi ndi losauka sikuti akumanena za ndalama zokha ayi komanso inu anthu okhala ku Malawiko ndinu osauka ndi nzeru zomwe. Tawonani ma comment ameni mukumalemba apa it shows kuti simukuziwa china chilichonse. Kumaonerera news zakunja chonde muwone anthu mmene amachitira ku SA, USA, UK, TZ, France, ndi maiko ena otere. Anthuwo ndithu sanalakwe it shows kukonda chipani chawo komanso kumukonda munthuyo chifukwa ndimusogoleri wawo ndithu therefore they have to protect him. A Malawi chonde dzukani mugona mpaka liti!
Nawesoo tikakwilirra kundata, umangova trison ukhaula ugwaso ngati m”bale wako uja
Koma guys dzikoli anthu enadi alibe ma plan eti? Zowona munthu ungamamujijilikire nzako mkumagona panja munthu oti akatuluka pa bail sakupatsa mmoni komwe chifukwa sakudziwa? Mutsegule Ku business page nyasatime yomweyi muwone momwe anthu akutsegulira ma company mu dziko lomwe muti sizikuyendali. Think postive in any problem you face. Ndimawelenga mafunso pa qoura komwe wina anafunsa kuti kodi kungakhale bwanji dziko lapansi atati anthu onse a below average IQ atati asamabelekane ndicholinga choti asachulukane? Yankho linali loti dziko lapansi litha kukhala dziko labwino lomwe anthu onse atha kukhala ogwiritsa ntchito mitu pochita zinthu. Zachisoni nzoti anthu amene amafuna adzigona panjawo… Read more »
stupid actions require anough tear gas. MCP can not go into govenment through the back door. USA and others amangobweretsa mpungwepungwe. ulemu ndiwofunika. Why are Malawians today angotukwana mosaganiza. Why can’t you bring solutions? A constructive MCP and a constructive USA can see Malawi achieve growth.
These are signs that the young kangwazi is about to go to Ndata to rest in ‘peaces’ the devil has already opened his doors to welcome him to the land of darkness. We will be there for a rapturous send off as Chilima will be taking over the reigns of power.
Almost everywhere in Africa the police are the cause of insurgence because of their overzealous conduct. They always growl like angry dogs even when what is happening is not worthy any salt. Remember the Chilumpha and Matumula “treason” trumped up cases, the DPP and the stupid police said they had overwhelming evidence and MBC went ahead to air the inaudible conversations and wasted so many millions which could have benefited Malawians? As if that was not shamefull enough the same DPP and police are at it again; MBC as usual, without shame, chose to air the purpoted doctored Whatsapp conversation,… Read more »