Email a copy of 'Malawi VP Chilima, MCP’s Chakwera, Manganya put under NIB surveillance: MBC blackout ordered' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Malawi VP Chilima, MCP’s Chakwera, Manganya put under NIB surveillance: MBC blackout ordered' to a friend
Malawi Bureau of Standards says it has instituted investigations after reports that a Chinese upmarket hotel, Peacock and Pacific Hotel...
Rubbish to which journalist is Kaliati giving this blame I think She must have forgotten, are they not the people in their party using MBC for their own political gain by denying the opposition to enjoy the benefit of the tax payers sponsored stations. Shame on you mai start by putting MBC in order then come and accurse the private journalists
Ndale zakuno kuMalawi ndi momwemu.ndingofuna ndikuwuzeni inu aDPP kuti ngakhale mutaipitsa mbiri za atatuwa ngakhale mutamukhomelera bwanji Chakwera koma ulendo uwu wa2019 mukutsala.mukudanaso ndimunthu amene adakuikani pa mwamba?ADAUSI limakukanikani dera lakwanu lomwe ndiye muli apa kubwitika amalawi opusa ndani angakuvereni?MBC timaidziwa kale kuti imalamulidwa ndi boma ndi cha zeru chanji angauze amalawi koma dziwani ichi 2019 ikubwera mudzasefedwa mosakuverani chisoni.nanji (aFiliph malonda) b ware.ok
this is malawi i know full of unprofessional spies who ends up in prededuce making pple hate one another,shame on u,God is there watching.
No wonder our country is living in 60s despite having clocked 53
kodi ku mw kuno tili ndi ufulu wacibadwidwe?????????????????????????????
cisoni zeedi. ndithu kumauza a malawi kuti mpaka muwaulula ndi zibwezi zao zomwe???????????????? cheap politics. nanga nde muyambe ndi pitala. ndiposo ose azibambo, akungika nkhope,amera mawerer, atukuka misana, akula zimimba, disproportion bodies ndipo azimai. ndikaesa ndalama zathu zomwe nzomwe zikucitidwa spin kumanyengerana, caponda sanakanidwe ndi mai ku embassy ku ethiopia???????? kucita kukwerera ndege??????????? ndalama zathu. osamangomwa kombucha yu bwa?
azimai ambili akucita secure ma position , kupeza nchito povulila mabwana knulandilaso ndalama. kukamba mwa mbwerera bwanji. osamakoza za citukuko.
muufuna mutiuzeso za BAKER TILLY mutibereso.mmmhui
those have tried to create udani pakati pa APM ndi Chilima is my pray that Satan should be put to shame your plans will not materialised in the NAME OF JESUS OF NAZARETH.
mavuto anu a DPP,don’t forget kut bwalo ilo ndilosiilana.
Dziko liri mmanja mwa agalu, the country has gone to the dogs, chalu chili mumaboko ya ntchebe. Thou shall not develop my mother Nyasaland.
Has MBC given MCP, let alone Chakwera, any platform? They prefer to publicise Chiefs and other hoodlums. As for Chilima, what DPP is doing is actually making him very popular. He does not need MBC platform. With regard to Manganya we still watch his show on other platforms. DPP is full of dunderheads and what they are doing are signs of panic. They are a very scared lot.