Email a copy of 'Malawi woman kills girl by inserting 30cm stick into her vagina' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Malawi woman kills girl by inserting 30cm stick into her vagina' to a friend
South Africa-based Malawian prophet Shepherd Bushiri of the Enlightened Christian Gathering (ECG) scored a giant legal victory on Tuesday when the Gauteng...
How bad must your life be for you to be able to treat a human life as though it has the same value as the life of a chicken?
We are cursed lot….
Apart from the killer the mother of the child deserves to be punished as well. Why did she leave the 3 months old child sleeping alone?
EEEEEH! Ndilibe mau sizinaoneke pa dziko lapansi koma ziliko ku Malawi, uwu siuhule ai ufiti uwu ndithu.
Ine koma ndingafune atandipatsa ndimulange ndekha then ndikatsekeredwe ineyo
Why was the child targeted in the first place? If there were differencies, how were they involving this innocent child to deserve this painful death? Koma mahule inu , kuli bwino muzingotsekeredwa basi athu osapemphera inu
Uhule wake nde wachambatu mpaka kukapha mwana.She deserves a stiffer punishment otherwise she must spend the rest of her life in prison
Ndili ndi zaka close to 50 koma sindinaveko zithu za nkhaza ngati izi. Inu a mabungwe (CSOs) bwanji simulakhulapo when things like these happens? Bwanji mumangoveka pa za ndale zokhazokha (kuti mupanga ma demo). Bwanji simuchita join ma cases ngati awawa? Bwanji simupereka ndalama zanu to speed up these cases? Nanga ma NGOs and UN agencies, Save the Chidren, UNICEF, “is this outside youryour mandate?” This woman must be brutally and urgently killed. Pakufunika quick justice apa, a Police atipatse ife timubaye chimtengo ku nyini kwakenso chitulukite mkamwa basi.
A point well made. CSO, UN Agencies, UNICEF, Women’s League , Ministry of Gender etc where are you. This should be a cause for national outcry!
Koma umbuli ndi kufa komwe apa achawa atani nkhani ya chisoni ngati imeneyo Achaea ikwakuza chani
Azimai nkhaza muzibweza . Palibe amadziwa za Mawa. Muzimuuopa Mulungu. Analipo anzanu a chewa ena aku Dedza. This makes me cry for the lost child.
MHSRIP
Mmmmm Koma hule wankhaza uyu mpaka kupha MWANA wamiyezi itatu mwankhaza choncho ameneyu pakufunika aphedwe nayeso pomugenda ndi Miyala shariah shariah