Email a copy of '‘Man of God’ arrested for sexual assualt in Balaka' to a friend
Loading ...
Email a copy of '‘Man of God’ arrested for sexual assualt in Balaka' to a friend
The United Nations Children’s Fund (UNICEF) on 1st April 2015 rolled out a national advocacy campaign with Airtel and the...
Imadya pomwe Ayimangilira… Munthu wa Satana ameneyo, chamba chili phwe phwe…..
ZAMUMTIMA ZAWEKHA.ABUSA GONDOLOSI UJA AMENEYU
Abusa abusa abusa kodi chikukuvutani ndi chani . Osaitana azimayi a mvano bwanji
Koma amenewo si man of God koma satana ndinyerezakezo komaso makolo ndiopusa pomusia mwanao ndi ochewa okuDowao
Abusa mwatani zoona mmalo motsogolera nkhosa za mulungu inu ndikumawononganso aaaa mwatani mukuyipisa dzina la ubusa. Mmmm shame to man of GOD
Makolo tiyeni tiasamale atsikana pakuona mayendedwe,mavalidwe awo anawa avale mopusa enafa tangokhala ndi mtima odziletsa sinzeru zathu zitengera chisomo pliz~pliz~azimayi tek dis enafe mtima umafuna chifukwa cha zomwe akuchita ana akazi mmakukamu koma timaopa ndende!
Anyongedwe basi according to section 163 mukuonjeza mabusa abodza inu
5 years in jail according to section 163 anyongedwe basiii
Abusa ena alibe uzimu, nanga mpaka mwana wawo yemwe?
AMENEYONSO NDI MULOMWE?