Email a copy of 'Manyozo should be removed as captain, Wanderers fans demand' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Manyozo should be removed as captain, Wanderers fans demand' to a friend
Members of Area 25 (Sector 7) Assemblies of God in Lilongwe last Sunday donated a MK 1 million cheque to...
Instead of fighting for welfare of players u are busy castigating them.
Ayambe pasuwa
achoke kae pasuwa!
a mponda valani boot mukasewere ino ndi nthawi yoti titenge league osati manyozo nosense
Kodi ku Malawi kuno bwanji ma Player kupanga Demand ndalama zawo ndikulakwa? Koma azingwira ntchito zaulele asayankhule ayi akayankhula alakwa aziopa..chonde nawo ndi anthu akungwira ntchito Ali ndi Ma Families nanu ma Supporter inu mukudya makwanu mukumanga manyumba ndalama zongwilira ntchito anthu ena nde poti akuzuzulani basi Manyozo ngati Captain sanalakwe ndichifukwa Ali Captain amayenela aziwayankhulira adzake ngati Tsogoleri iyeyo
Koma mpira wa ku Malawi ndi wauchitsiru. nanunso a Wanderers, with all the indiscipline Joseph Kamwendo had been associated with even the time he was captain, you never demanded that he gets stripped of his captaincy. It took Yasin Osman to take away the captains armband
ZAZII
zopanda mutu
TATIYENI TIONE KUTI MA GAME OTSALA TISALUZE AYI PLEASE PANO SIKHANI YOKOKANA AYI, KOMANSO IYE NGATI CAPTAIN NGATI ZILI ZOOONA SIBWINO KUTI AKUYAMBITSA NDI IYEYO IYE NDIYE OWAUZA ANAWO KUTI OSADANDAULA NDALAMA ATIPATTSA BASI OK KOMA ZONSE ZIMATHA NDIKUKAMBIKLA ZAKUCHIPINDA TILIMBIKILE BASI MWINA ANZATHUWA AKHOZA KULUZA MA GAMES AWO INU MKUWINA ONSE BASI NDE KUTI MULIBWINO KKKKKKKKKKKKKKKKKK ZABWINO ZONSE NYELELE