Email a copy of 'Maulidi claims backing from PP brass against JB ' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

35 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
kamps
kamps
9 years ago

Bena mphoto mose ndimwe vindere vyakufipo.nadi hule la chanakazi limupusikaninge, imwe nadi matongo lende kuti tiyeni tiyeni tiyime pathekha.aah ndimwe vizeleza!

Walhelha ochavo
9 years ago

koma ngati mulumana ndikudyana chenjerani mungapwetekane

John Chilembwe
John Chilembwe
9 years ago

If MEC failed,it was PP’s ineffectiveness on it as a state body.Funding was very poor,logistically nde worse,analephera kuwapanga empower mokwanila for tripartite elections.
Wina amati aMaulidi munangoti akhale pampando,basi kukanilira.Owowooo,kuterokoo.
Anaonera abiti maloko,nawonso kungoti khalani apa yiiiiii,mpaka kukanilira kutsala pangono kuyambitsa nkhondo.

Anthu tisamakonde kukamba za ena coz sitiakonda pomwe nafe tikupanga zomwezo.Taonaninso shadow cabinet ya MCP,koma bwanji kukuwa kwake ndi ya DPP.

Tiyeni tinene chilungamo pa chilichonse,sitimati God Fearing Nation.

Ntchisi boy
Ntchisi boy
9 years ago

PP first lost its vice president central due to political carelessness. The party was quick to dismiss him as lazy and useless. Then it lost its vice president south and then North. The party took it easy. Came elections the party got a third position and blamed MEC for that without doing any serious soul searching. Now the party is repeating the same blunders by standing on the way of the very people who want to hold up the reputation of the party on the ground through participation in the by elections……
Does this party learn from its past mistakes.

Manuel
Manuel
9 years ago

Pipii ! kenako odi uko! chipani chuukagwa! hutale siyuliranso odi uko!!!

Kapenandiye
Kapenandiye
9 years ago

Maulidi wachita boo. Asiye abiti lock ndikulephera kwaoko asati akuletse iwe. Iwo anapikisana analephera pa 20 May paja, iwe ndi ufulu wako kutero uwone kuti ulephelera pati. U don’t trust MEC because u failed. Ngakhale kukokerako no 3 iiiiiiii abale inu, ati mukati boma sililuza taonera inutu.

King of Israel
King of Israel
9 years ago

Maulidi pliz stop this unless if its a stunt

Mashino amingi
9 years ago

MAULID, MAULID, is a complete political FAILURE! He was in UDF, failed. In st. DPP failed. MChipani ndi boma la amayi athu, he failed. Then anangomukokera kuti akhale Acting SG ndiye akaupanganso makani. Inu, a PP Musiyeni ayime pa zisankho. Ndipo alephera. Koma chonde akalephera musamulorenso mu Chipani chatu. Akayambe chake ndi mzake failure wina ” his excellency Chenji goro Uladi Musa. president wa chipani cha anthu awiri. Asaaaaaaaaaaaa. What a couple!

Mbwiye
Mbwiye
9 years ago

Akunama amaiwo, a Maulidi kapikisaneni. Nseu wa Lirangwe Chingale mpaka ku Machinga kuti utheke pakufunika anthu ngati inu. Please do not give up. Ken wa chinkhope ngati nyani kapena amai oyenda ngati bakha sangabwelese chitukuko kwanu koma inu basi. Maulidi yemweyo koma kuti wa wa wa wa wa wa !!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!

Chetepa
Chetepa
9 years ago

Kayambe Chako chipani iweeee tione ngati ungathe!…pew pew pwe za ziiiiiii MEC ndi mbava Zokha Zokha we will never deal with that MEC unless we are idiots like you!

Read previous post:
Malawi govt justifies decision to defer Information Bill

Malawi Government through its Chief Information Officer John Chilikizo has defended government's decision not to table the Access to Information...

Close