Email a copy of 'MP decries rising poverty in Malawi: ‘Single digit inflation does not mean anyting to suffering citizens’' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'MP decries rising poverty in Malawi: ‘Single digit inflation does not mean anyting to suffering citizens’' to a friend
Zomba Chingale, member of Parliament (MP) Wallace Chawawa (People’s Party –PP) has said the micro-economic indicators that governmetn says were stable...
Can we even trust these single digit inflation figures? The evidence is not there. Good for her to speak up on behalf of her constituents: they elected her to do just that, but not many MPs do.
True, DPP is torturing us, chochita chikusowa abale, kukolora mbeu kusowa kokagulitsa, tipanga business yanji, magetsi kulibe, titani tsopano……..zinthu zikungokwera daily, mavuto okhaokha —-zamanyazi.
Mukunena zoona Mama.Anthu akumudzi tikuvutika.
Inu A Hon Kandodo Chiponda anthu akwanuwo ngati sakutuka ndiye kuti ndialesi olo nthawi ya mbwiyanu kamuzu alesi ngati amenewo analiponso ankalephera kutimiza anaawo ku sukulu ili k3.00 ( three kwacha )
Atukuka bwanji anthu atagula fertiliser k20,000 thumba chimanga mukuwagula ma k50 per kg. Soya less than k200. A NFRA akufuna kugula kwa big traders who can afford to pack a track.
So ulesi but inequality gap is too big.
Hear her, the daughter of Malawi,born from parents of credibility, you may be mistaken, it’s Chiponda not Cha oky.