Email a copy of 'Nankhumwa, Uladi promise to win more DPP seats in 2019 polls' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

15 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
Hatton
Hatton
5 years ago

DPP has assembled a formidable team. Uladi, you are the cream of central region. MCP yayamba kale kunjenjemera. I for one I am confident of your success in the region. The only criteria that MCP looks for one to become the president of the party ndi nkhanza. Kutereku amene akutsogolera kongilesi ndiwankhanza and soon he will graduate into a killer and start killing per MCP’s trade mark. Nankhumwa, you are indeed a star and we will make sure that this star continues to shine brighter. What is even more interesting is that you are younger than achinyamata olandawa omwe akuyambitsa… Read more »

Watson
Watson
5 years ago

MCP, chipani chakupha, chonzunza, chosankha mtundu komanso chonyoza ndikutukwana ngati m’mene akuchitira wochisapota ake pa social media

ANANVERUWA AKUMALOWA KWA MAGODI
ANANVERUWA AKUMALOWA KWA MAGODI
5 years ago

Akulu mulunguwache asamanyozekayo mukunena ndani m’bona yemwe amakhala ku khuluvi uja eti kapena mumapembeza mulungu wa ma HINDU uja amakhala m’madzi mu Ganges liver (GANGA MAA ) nanga inu mene DPP ikubelamu kuzunza AMALAWI chonchi wina anga manene kuti eeee mulungu sanyozeka watonyeredwa chani. maganizo amenewo unphawi sungakuthereni mwanva tisinthe tione zina basi CHILIMA VOTE BASI FULL STOP.

liwale
liwale
5 years ago

day dreaming

passportgate
passportgate
5 years ago

Corrupt party. Tilinanu mpaka kuthana nanu like mmene tapangira chaponda. Very promising under Bingu as a takeover. Nankhumwa and team know things change. Its not long we sha be talking of somone beating u

Kadzakumanja
Kadzakumanja
5 years ago
Reply to  passportgate

Kkkkkk

Banda
Banda
5 years ago

Komatu zinthu zina ndisoketsa eti, zoona a Uladi Musa angamanamize anthu kuti ali ndichikoka ku central region? Maloto chani,kapena kunamiza anthu eti, zovetsa chisoni.

Maunits
Maunits
5 years ago

Mbava izi tithana nazo 21 May 2019 zisiyeni. Uladi alindichani pachigawo chapakati. Munya muona mwatizunza nthawiyayitali kobasi. Nankhumwa go to Mwanza and sort out district council staff kulubwa lubwa basi who can vote nkhalamba lero fokofo.

Makanda Ntchembere
Makanda Ntchembere
5 years ago

A few months ago Uladi was being investigated on the issue involving passports and DPP made a lot of noise about it and his case is still in court. How different is he from George of Maize gate scandal? Is passport gate a lesser offence? or people are just attracted to the prince of thieves?

Tiyeseni Phiri
Tiyeseni Phiri
5 years ago

You feared Chaponda because he is a presidential material. Your interest is not to fight corruption. Your interest is to fight potential presidents. Shame!

Kadzakumanja
Kadzakumanja
5 years ago

Koma guys Chaponda akakhale presidential material? Olo ma donors kuona nkhope imene ija aid ingabwere?Muli chani mwa Chaponda chomwe munaona inu kupatula kunyoza atumbuka?

Nox Nthambi
Nox Nthambi
5 years ago

Uladi Mussa you have never achieved anything more just your parliamentary in Salima (I can’t even remember the constituency). Your track record in getting results is very poor tracking back when your in UDF, DPP (under Bingu) and PP. Can you offer anything new to attract eligible voters in central region. I doubt. The simple word(s) that fits you is that “You are a failure Period”. Tg=he greates mistake that DPP made is by choosing this former Madras Teacher as VP for Central Region.

kels
kels
5 years ago
Reply to  Nox Nthambi

Lol… ma dotolo akhazulidwatu ndi aphunzitsi ak madalasa..

Samuel
Samuel
5 years ago
Reply to  kels

Mulungu akasankha palibe angalimbane naye. Osathamau aliyense alipanzera. Uwu ndimpikisano. Amene Mulungu amusankhayo tidzamuona pa 22 May 2018. Osanyozana amalawi palibe amapambana pamene mpikisano usanayambe. Mudzakhumudwa. Mulungu sanyozeka.

Tiyeseni Phiri
Tiyeseni Phiri
5 years ago
Reply to  Samuel

Musamunamizire Mulungu!

Read previous post:
Joyce Banda turns up heat on Mutharika: Asks Malawi leader to respond to resignation calls 

Former president Joyce Banda has added her voice to calls for President Peter Mutharika to resign to allow those who...

Close