Email a copy of 'Nyasa Bullets find Airtel Top 8 final signal: Malawi champs Nomads in crisis' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Nyasa Bullets find Airtel Top 8 final signal: Malawi champs Nomads in crisis' to a friend
Divisions have erupted in the leadership of the Evangelical Church of Malawi over a pastoral letter scheduled to be read...
Ngati kuli dziko lower anthu ake ndi a uve ndi Malawi. Chifukwa chosangalala ndizigoli za mpira mpaka kuononga stediumu ndi Ufa kapena penti. Munawaona anzathu kujoni ngakhale amachmerera mpira mkati koma zauve ngati izi panalibe. Anthu ena munabadwa opanda dongosolo mmakhomo mwanu mukuononga dziko, mukuononga ma infrastructures
Inu musamayankhule ngati kuti mukuyankhuza zithu zazeru. Kujoni mukunenako munazimvela kuti zaboza ngati zimenezo. moti inuyo zimuziwa kuti Mkaka ndi mazi?
A neba pepani next time. Munapanga phuma first half munaiwala kuti Bullets ndiku madzulo