Email a copy of 'Peacock donates seeds for winter cropping to Salima farmers' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

5 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
Mayo
Mayo
7 years ago

Nanga iwe nzanga Bwande udamvapo kuti Chakwera kapena Jessie kapena Msowoya wagawapo zinthu zaulere? For Msowoya zomwe ndinamva ine ndizoti adathawitsa chibwenzi chake Jessie Kabwira ku Parliament kuti asamthire nawo unyolo penanso ndidamva kuti adamtuma nfana wina wake kukaba ” mfuti ” ku Capital Hill basi!

Bwande
Bwande
7 years ago
Reply to  Mayo

Tiyeni nazoni. Sikuti ndizolakwika. Koma penapake pakundiopsya makamaka zomaona kuti mtsogoleri wabwino ndiye kuti ndiamene akugawa zinthu zaulele. Komabe popeza ndimmene tinadziwira democracy yakwathu kuno. Atcheya anawononga zinthu. Ukuwona bwanji bwanawe

Nduma
Nduma
7 years ago

Apa pokha pastor Chakwera sangamake. Jumbe ndi mitunda ina iyi. MCP cannot defeat him.

Mayo
Mayo
7 years ago

Koma man Jumbe ku MCPko kukanakhal anthu anzeru ngati inu atatu kapena asanu chipani chanucho sibwenzi chikuchititsa misonkhano kwa anthu kuchuluka kwake ngati a pa maliro a munthu opanda kwawo.

Bwande
Bwande
7 years ago
Reply to  Mayo

Chifukwa chakuti akugawa zinthu zaulere?

Read previous post:
Ruling on Mphwiyo shooting case set for end June: DPP Kachale tussles with Kumwembe

The Lilongwe High Court has set the last week of the month of June as the tentative day presiding judge Blantyre-based...

Close