Email a copy of 'President Mutharika consoles Muluzi, Busile: JB sends condolence message' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

24 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
Betland eziben
Betland eziben
7 years ago

R.I.P Nthawi zonse ndife maluwa. Ndipo sitimatha kuziteteza Allah adapeleka chisisi chomwe mwini kuzindikila ndi iye ife kuziteteza kwathu ndikulira. Ndikupempha makomo onse aku jaanah asegulidwe. Pamodzi ndi onse omwe atisiya munga abale ku chipembedzo. Mulungu Allah akuyikeni kuzanja lakumanja inshaallah manda anu akhale nulu yowala nthawi zonse Ameen

chindere
chindere
7 years ago

a Joyce Banda kundondela bwanji? Why only condole one family? Ndimayesa pali mabanja awiri amene ali a nnamfedwa. Stupid politicians thinking yawo ndi imeneyi. Anthu wamba like samawaona ngati kanthu. Iwowo is about pleasing fellow politicians. Amayi onamizila kupemphela amenewa. Mayi wamvano apepesa banja limodzi lokha when there are two bereaved families

opinion
opinion
7 years ago
Reply to  chindere

Chindere, maybe the name befits you! Why blame Joyce Banda? Has the president also gone to condole the other bereaved family? When the tragedy happened, Nyasa Times also concentrated on the death of Muluzi’s daughter it was not mentioned that the other lady had also died although it was indicated that both had been struck by lightning. That is the way things are – If you are a nobody in life, your death too will not matter!

Shantal
7 years ago

Pepani kwambiri

BigMan
BigMan
7 years ago

He wore a black tie. It doesn’t have to be a black suit.

rennex bamusi
rennex bamusi
7 years ago

its so sad and May their souls rest in eternal peace.

blessings
7 years ago

Pepani akumabanja onse awiri chifukwa cha zovuta zimenezi zomwe zatigwera, mulungu atithontoze tonse pamodzi ndi mabanja ofeledwa.

Daniel Hussein
7 years ago

Rest in peace

betty mlenga
betty mlenga
7 years ago

Pumani bwino…kwathu si padziko ndingopitilira AMEN

Bob
Bob
7 years ago

Umati avale chiyani ndiwe foreigner wakuti ma be Tanzania ,kape

Munthu wakumudzi
7 years ago

Petulo you are so stupid ngati chonena chinakusowa kuli bwino kukhala chete. Iyi ndi ngozi palibe amene anakonzekera ndipo izi sizandale ai. Kodi apa waonapo mbendela ya chipani? A president akonso palibe chimene anakunanepo ai ali pwii chonsencho ndi mbusa. Stupid kagwere uko, shatapu.

Mawa ndiwe
Mawa ndiwe
7 years ago

Zakhudza Chakwera why? unava kuti Petulo ndiwa Chakwera? ndikwanu komweko!!! ndi umbuli wobadwa nawowu mungatani? Leave Chakwera alone please!!!!!

Read previous post:
Malawi secure K16bn loan from African Development Bank for youth agribusiness

Government of Malawi and the African Development Bank (ADB) Tuesday signed a loan agreement amounting to US$22.4(MK16.5Billion) to finance the...

Close