Email a copy of 'Some primary school teachers  storm Capital Hill over promotions' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

13 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
Bob
Bob
5 years ago

This is a useless government.Stagnation is not only in teaching service but almost all government departments. People are retiring, some passed on and others left without replacement. Its only in few selected areas that people arebeing promoted and only after checking who is who.

Godfrey w. Nantali
5 years ago

Nanunso apolisi mwangoti chete osayankhula , ndalama zimakukwanirani? Nyumba zanu ngati za asin’ganga , ayi ndithu mwina mukusangalala nazo. Ubwino wake mwayamba chitukuko chokuza nyumba zanu ndi mablockboard , mmakhwana apolisi athu.
Mukamatchedwa migwanya mmasangalala eti. Anthu ofunika padziko pano, ena mwaiwo ndinu Apolisi athu , komanso Aphunzitsi , koma zachisoni boma liribe nanu ntchito , ndiye come 2019 muzaziwe chochita , osati muzingolira , mulira mpaka liti ? Nthawi yakwana muwapase phunziro anthu amanewa , inu zoona K100, 000.00 masiku ano ndichani ? Mwakula mwatha muziona nokha.

Emarire vava
Emarire vava
5 years ago

Kodi anzathu a DPP simupangako Ka comments nka modzi komwe? Moto wakupalirani Saulosi uwu. Every day amaitokosa nkhani ya ma promotion a ma phunzitsi

JJ Mbewe/pathfinder
JJ Mbewe/pathfinder
5 years ago
Reply to  Emarire vava

Ndiye ndipamene ungadziwire kuti ife a DPP tilipo ambiri. Nkhaniyi ili ndi ma comment ten okha. Kuchotsapo a ine wa DPP anga awiri, patsala eight and that is kuphatikizatu zipani zonse zotsutsa. Koma tikanakhala kuti tonse a DPP tinachita comment bwezi pano chinambala chiri pa hundred (100)

Thyolo Thava boy
5 years ago

Go teachers go akupatseni zanu, asamakhalire kugulira anyamata mowa, press him kaya agulitsa magalimoto achipani okuba aja kaya , kaya atenga MK145m amanama kuti abweza ija asova. Go Go Go teachers

Kanyimbi
Kanyimbi
5 years ago

Paja a Bamusi akuti zopepera zikuchitikazi ndi Ngwazi APM akuchita kkkkkk osati nduna.

JJ Mbewe/pathfinder
JJ Mbewe/pathfinder
5 years ago

Kodi nanga abale, kukwezwdwa pantchito umachitanso kuopsezera bwana kuti akutero? KKKKKKK anthu awa ndi ajatu amanyemera bwana kuti akwezedwe pantchito, koma panopa chifukwa chakuti ndi boma la DPP lomwe ngakhale ndi utitiri omwe ukumveka bokoso lake, anangoganiza kuti akathamange kunseu.

CitizenX
CitizenX
5 years ago

Good timing, if you have a problem with govt this is the right time to make your demands if you are serious about making change in your life, Election time is here kkkkkkkkkk. SO WHO WILL BE NEXT??????

mkhonde mwenecho
mkhonde mwenecho
5 years ago
Reply to  CitizenX

That is the way to go now,get united and pressurised the government till you get promoted

Change is needed
Change is needed
5 years ago

Inu 4 billion kwacha yomwe mudawapatsa aphungu chifukwa chokana ma electoral reforms aja, zikadatheka kuigwiritsa tchito pa aziphunzitsi anthu. Khalamba zopanda manozi abale. aziphunzitsi mudziwiretu akangowinanso ameneyu mwanya. Ndalama m’mene zikupitira ku America komwe kuli ana ake chikhalirenicho tidavutika ndife kuvota. Ana ake sadavote nao koma akungodyerera.

HoRror
HoRror
5 years ago

Tikuyandikira zisankho, nayeni maliseche. Pano chilichose nchotheka sangapangeso ngwingwingwi akupasani ndalama zanu.

Jimmy
Jimmy
5 years ago

Maliseche’s days are over now.phunzitsi kumtero?

Read previous post:
Police recovers car stolen at Chinsapo taxi rank,  suspect arrested

Malawi Police in Lilongwe have recovered a stolen vehicle Toyota Sentra Registrationnumber BV5033 which was stolen at Chinsapo Taxi rank...

Close