Email a copy of 'TNM writes off Bullets K10.3 million CAF debt' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'TNM writes off Bullets K10.3 million CAF debt' to a friend
The Balaka First Grade Magistrate Court in eastern Malawi has sentenced a 23 year old-man to seven years imprisonment with...
Ife Ndife Amwai,enanu Mukakondwa Ndiye Mwachinya Bullets,ife Kukondwa Mkosatha Coz Ndalama Zimangochucha Ngati Mvula Mumlengalenga.
I’m impressed with the gesture by TNM. However, comments 29 and 40 are bad to the taste, not good for football. It was not written that BB will never land a sponsorship. Both of you are not prophets (if any then you are false prophets) to prophesize BB’s future. As a matter of fact let me assure you that as long as we have the living God, BB will surely land one sponsorship, a hefty one for that matter.
Inu ATNM inu simunapange bwino ngongole ndi ngongole palibe kuchotsela osamakhala ndi mtima okondela team coz apa zawonetsa kuti muli ndi side bwanji ngati ndikukhulukila ngongole/ngati ndalama zakuchulukilani mugawe kwa each team osati team imodzi mateam ambiri ali ndi mavuto akulu akulu kupambana komwe mwathandizako ganizani bwino ife timakonda masewero ampira koma Network yanu
TNM KNOWS THE TRUTH IN THE FIELD OF PLAY AND WAS OBSERVING THE MATCH SESSION AND SAW THE BIAS OF THE COACH AGAINST THE PEOPLES TEAM AND FELT PITY FOR US. HENCE THE CONSIDERATION. THANKS TO TNM. GOD BLESS YOU ALL AND SHOULD CONSIDER YOU.
TNM ayiwelengera patali kuti bullets cingakwanitse kubweza debts minyama yachuluka eee!
Bullets team ndi ya a NAMFUKO osati team ya fuko. Fokofo zanu mudzakhala olira komanso osauka mpaka muyaya. Matama musiye, mwano muleke. shupiti zanu nonse a mauleeeeeeee.
Koma ndiye saporter mapeto abebatu sindingayinve na zokha mwaangazi a TNM mwaitha ifenso tikupangani konzu!!!
Mukuwonatu! BB cows cerebrating, Kkkkkkkk bb team ya minyama!
MORE THANKS TNM….ZIMENEZO NDIYE ZA MPIRA….Ndiye muwone mmene titawaphulitsire matimu enawa mu second round mu….BIG UP Once again TNM
A TNM apangira dala kukhululuka ngongole chifukwa choopa mnyozo, iwowa ndi amene analepheletsa AIRTEL kuti iwathandize nthawi imene amamenya CAF ija, mix kuluza kwa Carlsberg cup angoti pasavute a Bullets asafe kwambiri, chifukwa malingaliro awo anali oti Bullets will win so that they will be able to repay them .koma eeeeeeeeeeee Dzanja la yehova likalemba lalemba basi.