Email a copy of 'Uladi says ‘Mutharika must fall’: Slams ‘clueless in control’ DPP' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Uladi says ‘Mutharika must fall’: Slams ‘clueless in control’ DPP' to a friend
The High Court in Blantyre is set to hear a judicial review of a case where two directors of a...
Inu a Kabwira, banja linakulakani. Munganene chani chopanga anthu ma million kumva. MCP kwathu ku KU timaikonda kwambiri, koma inu a ku Dedza ndinu munadetsa chipani chathuchi, lero muti chani. Kulephera kupanga reconcile ndi munthu mmodzi koma apa nkumati a Malawi, a Malawi ake ati? ife ai. ma bukhu munamwera, koma ndinu mbuli mkabadidwe. Ma disasters onse aja inu mkumati fwefwefwe, ngati ife timakhala ku Zambia kuti muzitilongosolera. Pitala amapanga mvula? Kanamizeni ena, osamangoti amalawi amalawi, za ziiiii ife ai. amuna anu akuti mukambilane, mulere ana apa.
Imwe ndimwe yai, a Kamlepo, a Uladi, a Mkandawire, imwe Chiuta nga wakamtolani muchali twana. 1. u r are useless politicians Malawi has ever produced. 2. Mose ndimwe tuntchewe uto tubwenhta kutali na chimbwi. Pala munazeru amalawi wakatikana uli. u have empty long speaches. kwali ma advisers winu mbambula zeru nga ndimwe. To hell with our PP
Koma zinazi kumangoziona basi
If Malawi was an established democratic entity,Muluzi could be put to task for imposing criminals in the country’s top leadership.All the shortcomings we are seeing today,is the responsibility of former President Bakili Muluzi who took the torch to campaign for Thom Muthalika whom he had no clue of the rogue’s characters or political standing.In his UDF,there were some highly competent leaders like late Aleke K.Banda and Chimunthu Banda (no relations) who could one of them,run our country diligently and patriotically.Bingu then had been fired from COMESA,for stealing US$475.000 in public funds.His brother Peter,was also in dire problems with Washington State… Read more »
lipenga inunso ndi phwala lamunthu ndithu I don’t even think kuti lipenga lake limalira how could you evolve bakili on this? forget that chakwera adzalamula dziko lino. what happen to jonah when God told him kukalalika ku nenevi? anathawa but It took God himself to put him on straight line soon God will put chakwera on straight line to go back to preach the gospel not what your saying zoduka mutu apazi.
DPP WOYEE!!!
No matter how and u may try how, it ll not work for u. MCP have u forgotten how u mistreated malawians for 31years in power? What is the problem with u? Jealous, let Mutharika alone to rule the country, agologolo inu machende anu, mufuna mubweretse chisokonezo mdzikomo. Amalawitu atopa nanu mukuona ngati mungadzalamulirenso dziko. Akhale wachilungamo chatsika wanuyo akanathawa ntchito ya Ambuye. He is a cursed person coz is aman running from God.Chilungamo chili ndi Mulungu osati anakafumbwefumbwe. Mudzichita utsiru wanuwo ku Lilongwe komweko. PP ili ndi fungonso kkkkkkkk sikusowa mbalume kumeneko mpaka kufuna friendly ndi leadership. Amalawi asakunamizeni… Read more »
peter yemweyo kuti wawawa!!!!
Uladi woyeeeee PP woyeeeee. …. Press harder and harder in so doing we can survive.
I am not a supporter 0f DPP, but nobody will give a chance to PP to rule this country again. The cash gate is enough material to us to reject you no matter what you say against DPP – your Msowoya Msowoya knows this. Everybody has seen that you are power hungry and please tell Kabwira and her party that they will remain in the opposition for ever because we all know how power hungry you are and we know when you get into power, you will be filling your pockets first. Let those people that have already filled their… Read more »