Email a copy of 'UTM will hold elective convention – Chilima' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'UTM will hold elective convention – Chilima' to a friend
Minister of Home Affairs and Internal Security, Cecilia Chazama has described the construction of new cell blocks at Maula Prison...
Kodi anthu mukavota kuti. U have results already of 2019 election. Wait ask mai Banda malawian are unpredictable
Attracting huge crowd? So mukuganiza kuti anthu onse akupita ku minsonkhano kwanuko adzavotera UTM. Ife a Malawi ndi khalidwe lathu kupita kulikonse komwe atipempha kuti tipite. Ku chalichi, ku misonkhano ya ndale, etc. timapita mwa unyinji. Anthu tikumapita ku misinkhano ya MCP, PP, UDF, DPP. Ngati mukuganiza kuti uyu wa matama uyu adzawina mwa uponda. Muwuzeni apange resign tiwone ngati anthu adzapekezenso ku misonkhano kwakeko. Akukamira chifukwa chani. Nayenso ndi mbava yokuba akufunika ma legeni akutibera ndalama zathu. Sitinamuvotere kuti azipanga twitwitwitwi ma sireen kupita ku misonkhano kukacheza ndi Calista ndi Patricia. Fotseki!
Time out no point. Even the other parties are doing that. How do you know what is going to happen. Pumbwa wa DPP iwe.
Foolish gwaragwara iweeeee, u r blinded by evil sprits. to hell with stupid ideas.
Surprise, surprise. Why should the manifesto come before a convention? Who made fundo zimene UTM is outlining during its rally? Chilima? Is this not putting the ox-cart in front of the oxen? I think apa zinthu sizinayende m’mene zimayenera kukhalira. It is the party convention that sets policy guidelines of a political party. I think UTM needs to accept that they should have done better here. In democracy, it is people that are elected at an elective convention that are expected to decide on issues that need to go in the manifesto. One person cannot sit down and write a… Read more »
Mulibe zones…phalani chats…just copy and paste texts
Chilima is creating good excitement. But Malawians beware the same people who created the DPP we know today yakuba ndi kupha are the ones behind Chilima. Kaliati, Masangwi, Mulli and Callister. I am sorry but my vote will not be for UTM come May next year
CHILIMA IS GOING NOWHERE
Ulibho mfana chilima ndipo nzakuvotera but upite kwambiri m’midzi kuti udziwike kwambiri coz ngati sutero mapeto ake zizakhala za ku Zimbabwe zija m’ma taonimu aaaaa olo usapitemo kaye wawinamo kaye
How will the delegates be identified? Just thinking aloud!