Email a copy of 'When Crime controllers become Perpetrators: Malawi situation' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'When Crime controllers become Perpetrators: Malawi situation' to a friend
Multi-choice Malawi, the sole provider of Go-TV has spent about K3.2 billion on four towers the company has constructed in...
Dislocation of economics compromises integrity and patriotism. Oooh my foot!
THE MUST READ COMMENT. wapolice akulandila 45000, akukhala ku rent ku area 23,24 chifukwa mu line mulibe nyumba. Daily akulipila transport, nyumba akulipila 15000. Azichotsapo ya lunch, achibale akufuna chithandizo, ana akufuna school fees. Bolaso amene akukhala tinyumba ta police tonyasa chifukwa nditaulele komaso tili pafupi ndi police ndiye amakadya kunyumba. Wapolice opanga rent mtawuni komwe angakhale ndi ku Ghetto basi coz ndikomwe manyumba amatchipa. Ku ghetto komweko ndikomwe kumakhalaso ma Gamba ambiri ndiye wapolice angagwile ntchito professionally? Salary ukuthela rent, kulpila ma bills, transport lunch ku ntchito basi ya chakudya pa nyumba, fees, kuthandiza ma dependants kusowa, ukukhala ku… Read more »
Thats what hapens when u dont motivate ur workers by giving them the required insentives. For example, a police man is sent to Zalewa roadblock without food and then a lory full of chamba passes by offering 100pn the officer what can he do when the service has not provided ration at the camp? Timaziputa tokha zinthuzi aboma. Wapolisi akukhala kulend ndimarobbers do think angawagwire???? akhala neba otani pamalopo poti amati kumakhala bwino ndi anthu oyandikana nawo nyumba.
Zachamba.
Kukhumbana basi.
These are just few out of many reasons. Another one is these improper promotions. What will these uneducated bosses contribute? We have not seen much change thou. Angofuna alemele mwachangu. Tawonani ku traffic, CID
God bless the one who wrote this article. Seems lyk apolisi alibe owalankhulira. So much risk pantchito yawo yet with no motivation. Look into this, and the sooner the better.
CommentYes, good pay is a requirements at any workplace.But in Malawi pay go with qualufication; Diploma, Degree, Professional certificate of 2yrs training not 6 mths. So lets spend to train our security people to have required stds. GOD GUIDE ALL.
Too bad
The reason is not salary. If it were salary then all junior police employees would be thieves. SOLUTION: effect departmental transfers for all policemen/women every two years. Someone has already said that some police departments are at an advantage