Email a copy of 'Malawi Police intercept 35kg heroin: Drug peddler arrested' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Malawi Police intercept 35kg heroin: Drug peddler arrested' to a friend
Democratic community policing, crime and gun control are areas I have tirelessly worked upon for years as a resource to...
How many Chinese have been arrested for ivory deals?They are all over in villages nowadays looking for precious stones and nothing is happening lying to be in some cheap cloth business..Umphawi wavuta pa Malawi.Nanga munthu modzi wa cashgate amasunga billions yekha and how do you expect the economy of Malawi to tick like this?Mavuto afikapo.Aliyense akuyang’ana chimene chingamuthandize.
Alandire chilango moyenelera coz pofuna kuzitumiza mobisapo,amaziwa kuti akulakwisa.
Asakatulukeso ameneyo mukunena zowona
Good job to our police
We are not the fools in this country.
Amalawi mumamusuleni munthuyu.kodi simukudziwa kuti umphawi ndi ulova ndi umene ukumatipangitsa kuti tipange zonsezi.chinanso tikumaphysa mtima tikamawona a President ,nduna,ma mp ndi anthu olemera akumaba komaosawagwira.
He is a good man, he has not stolen someone property,
hes just trying to make a living. cashgaters ruined this country for the rest of us. cant you just forgive the guy?
A Muhamad?
Dzina limeneli ndi la sataniki
Mubwiritseni nyasi zakezo afe pompo asakatithere nsima ku ndende.
Uyuyu apita ku ndende koma akanakhala mu Nigerian akanapanga zimenezi akanangomupanga deport basi.