Email a copy of '2019 time for Malawi youth to put the ‘nothing for us without us’ motto into action' to a friend
Loading ...
Email a copy of '2019 time for Malawi youth to put the ‘nothing for us without us’ motto into action' to a friend
Minister of Information and Communications Technology Nicholas Dausi, who is also government spokesperson, on Sunday disclosed that the ruling Democratic Progressive...
Bvuto lilipo kwa achinyamata ndikudzikayikira , titha and tikhodza kulamulira ,chowawa ndichakuti timalira ndi ulamuliro wa khalamba zomwe zakhala zikutilamulira kwa nthawi ysyitali pomwe ife achinyamati sitifuna Ku onetsa kuti kwakwana kwakwana. Chonde achinyamata amzanga mphabvu dzili m’manja mwathu kusitha dziko lathu.
The biggest problem with most of the youths being elect is irresponsible..ndi angati achinyamata omwe akapatsidwa mpando in the public seats retain it at the next election?
First achinyamata akuyenera kuphunzitsidwa kaye bwinobwino rather than just supporting them to contest coz zimapangitsa anthu ena even their fellow youths to lose trust in youthful leadership with what they do when they are in power.