Email a copy of '9 judges at Supreme Court hear Khato case on Lilongwe-Salima water project' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

10 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
Ndapita
Ndapita
5 years ago

In South African parliament yesterday…..read

Thus, the firm Khato Civils had to retrench nearly 1,000 workers earlier this month.

Mboweni said: “The project, which began with a budget of some R40 million, has now escalated to something of R4 billion. We can’t have this situation, there is something wrong.”

Ndapita
Ndapita
5 years ago

Tsagulani mmaso ammalawi. Muzaombela mmanja mfiti zikumvina. Anzanu ku South African achimina ndi song a zomwezi zokhudza Khato civil. https://ewn.co.za/2018/10/25/mboweni-giyani-water-project-a-cesspool-of-corruption

Mtima uwawa
Mtima uwawa
5 years ago

Koma ziko lanthuli ndi chani OH God bless malawi. Nduna zomakana chitukuko choti chitukula ziko LA malawi mumaganizapo bwanji ma lawyers amakhala ngati sayenda mayiko ena,,, please guys let’s fight for malawi think about the coming generation azapeza chani mu ziko LA malawi, palibe nkhani yoti ndikuyitengera ku court apa. Ndantha ine mtima uwawa…..

Americano Hiwa
Americano Hiwa
5 years ago

Pathfinder, Please wise up. Malawians have learnt to insist on following procedures in government dealings to protect government money. Greedy politicians have used the thinking of your kind to bluff Malawians in the name of chitukuko with a hidden interest. One case is that of gensets, Zambia maize etc. All these projects usually sound too good, but if not transacted following all procedures and requirements, money is lost in the process. Government is just supposed to design and initiate projects within the armpits of the law. Period.

pathfinder
pathfinder
5 years ago

Ndimamva kuwawa kwabaasi when gulu lina la anthu likamatengera ntchito za chitukuko ku court, especially nkhani ya madzi iyi. You are denying poor people the opportunities of having good water. Mtambo, Kajoloweka, Trepence and MCP ya Chakwera, ngati ndi ndale, mudzalira mokweza. Kafunse zomwe zinamuchitikira John Tembo anakana nkhani ya chitukuko ku parliament chisankho cha 2009 chiri pafupi. Analuza mochititsa manyazi.

Bingu wa Mutharika
Bingu wa Mutharika
5 years ago
Reply to  pathfinder

Ikanakhala kuti project imeneyo ndi ya ku Mzuzu sibwezi agalu amenewa akumapanga zoterezi ayi

Fatchness
Fatchness
5 years ago
Reply to  pathfinder

Sure feels good to throw chakwera into the mix to ensure u pander to the minds of the ignorant….

sooosa
sooosa
5 years ago

guy madzi ndi moyo please bwwezi zili pena bwanji kodi a Malawi

Kaka
Kaka
5 years ago
Reply to  sooosa

Amalaawi mwapanga bwanji. Madzi ndi Moyo. . kapena mufuna chakwera or SKC akhale ma contractor. Anthu openga mwapanga bwanji

Read previous post:
Bullets eyeing Masters’ Babatunde ahead of CAF participation: Nigerian stars in Malawi football

Nyasa Big Bullets Football Club have allegedly gone into talks with Masters Security Services seeking the signing of Nigerian striker...

Close