9 Malawians feared dead in Tanzania accident

At least 50 people have died in an accident that happened around Changalawe in Tanzania Wednesday.

Tanzania accident
Tanzania accident
The accident
The accident

According to information reaching Nyasa Times in drib and drabs, the 50 include 9 Malawians who are feared dead in the accident which involved a heavyweight truck and a travel bus.

The bus was travelling from Mbeya to Dar es Salaam.

The Malawi government is yet to comment on the development.

Nyasa Times will keep you updated.

Follow and Subscribe Nyasa TV :
Follow us in Twitter

45 replies on “9 Malawians feared dead in Tanzania accident”

  1. Boma..please help us we need info & names, its really very scariy to travel to TZ nowadays lets do someting people- timakwelela kuvutika komweko zimabus za TZ koma it could have been better tikanakhala ndi yathu ya lokolo! issue ndi speed lets do someting please!!!!!! aaaaaaaah!

  2. Ma team athu nthawizina mumakonda kupita pa bus kumeneku. Plse zawaonekera a business zisadzakuonekeren. RIP those involved

  3. Can government start its own bus company to ferry people. These Tanzania drivers are very careless. I have been on these buses. The speed is horrible!

  4. munali amalawi ambili mmenemo okafuna ntchito kutanzania. 9 ndiodziwika ndi boma koma udusa mwachidule ndi oposa 9. zopasa chisoni .

  5. Anthu mungoti RIP koma ndi ndani amene afawo. Plse Govt do urgently inquiry on who have died. Ma Tanzanians are very careless in driving. They dont care. Ife a business timapita ku Tanzania to import goods in their buses kuti nanga titani poti kuno ku Malawi kulibe ma bus athu athu opita ku Tanzania kukagula katundu otherwise its a risk to travel in their buses. They cruse at unbearable very high speed. Plse Malawi have talks with the Tanzanian Govt to have proper rules so that buses and trucks be driven on reasonable speed. Its high time these 2 govts to do something. A business tili pa chiophezo ndipo tili ndi mantha kuyenda pa ma bus a ku Tanzania. Pafupi pafupi ngozi ndipo bus ya Tanzania ikapanga ngozi ndi chipere anthu amafa ambiri zedi. Anthu amapita ku TZ Kuti nanga atani poti kokatenga katundu wa kunja ndi kumeneko. LORD HAVE MERCY. A Muthalika ndi Kikwete panganipo kanthu chonde.

  6. Palibe ndege zoyenda pakati pa Dar and Malawi abare mpaka pano ??

    Maulendo a ma BUS ndi magalimoto sakudalilika kweni kweni Aaaa !!!

    TIKUTAYA MIYOYO YA ABARE AMBIRI PA MUSEWU

    MAY THEIR SOULS REST IN PEACE

  7. koma pena kumakhala sensitive with pictures from a fatal accident scene mweee may their souls rest in peace

Comments are closed.