A Nankhumwa abweleranso ku court: Ati sanakondwe ndi mmene anawachosera mu chani cha DPP

Yemwe adali wachiwiri kwa mtsogoleri wa chipani cha DPP kummwera, a Kondwani Nankhumwa, watengera chipani cha DPP ku bwalo la milandu, kutsutsana ndi kuchotsedwa kwawo m’chipanichi.

Let it sink in all Doubting Thomases that I, Kondwani Nankhumwa, have finally decided to give the DPP presidency a go

Malinga ndi owayimira a Nankhumwa, a Wapona Kita, a Nankhumwa adachotsedwa m’chipanichi mosatsata malamulo.

 

A Kita ati nkhaniyi idzamvedwa ndi oweruza mlandu ku bwalo lalikulu la milandu a William Msiska pa 12 mwezi uno.

 

A Nankhumwa adachotsedwa m’chipani cha DPP chifukwa chokhala nawo komanso kutenga mbali pa msonkhano wa komiti yayikulu ya chipanichi, NGC, omwe chipani chidati udalibe mdalitso wa chipanichi.

Follow and Subscribe Nyasa TV :

Sharing is caring!

Follow us in Twitter
Read previous post:
Chimbota CDO to raise K100 million for hunger-stricken families

As one way of raising funds for the hunger-stricken families, Chimbota Community Development Organisation, has organised a fundraising big walk...

Close