Email a copy of 'Chaponda defamation case against Times newspaper adjourned: Defence not ready' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Chaponda defamation case against Times newspaper adjourned: Defence not ready' to a friend
Some Malawians have taken to social media to question Prophet Shepherd Bushiri’s deafening silence on charity works. Prophet Bushiri has...
May be they should change the name from MCP to another one. As the label is still MCP people will still be shivering at any mention of it. Mukuwonetsa kufatsa panopa chifukwa mwayi wolamula mulibe koma any mistake yolora inu kulowa m’boma Youth League idzatuluka from nowhere mwinanso before official results. Uniform ya red and khaki zili thoo m’ma suitcase. Kulephera kasanu kwa chipani chachikulu ngati chimenechi ndichinthu chokhumudwitsa kwa masapota. The history of the party is still in people’s minds that is why when a polling day comes many voters remember the party’s history and vote it negatively. Chakwera’s… Read more »
The Good thing is that people know that Times Group is used by MCP to push for its agenda including kuipitsa mbiri ya Chaponda. Nation newspaper is the best.
Kodi a Kongolesi ndinu otani, mwayamba kale mantha bwanji? Nkhani siyinalowe nkomwe mu Court, zitsiru za wanthu inu, a party of death and darkness. What I can tell you is “you can’t delete history” any attempt to erase history becomes history itself. Don’t we read about zimene ankhachita a Roma during dark ages, don’t we? Nde why should we not talk kuti ndinu akupha? As far as am aware simudzawina nso chisakho, I swear. Muzingolira kuti atibera mayooo!!!! chisakho chilichinse unless you resurrect anthu amene munawaponya ku ng’ona aja. Mbuzi inu, mabatile anu.
Aputa munthu olakwika. George Chaponda from Yale University. Madalitso Mussa ndi anzake anye manyi sopano
George Chaponda akupita kumapeto andale zawo akufuna Court liwavere chisoni koma ACB musamusiye ameneyi ngwakuba Times sinalakwe ,komanso a DPP anamugula Kenyatta NAYIRENDA
Anthu amenewa anamuipitsira mbiri Chaponda they have to pay for their professionalism
Eiiiiiish, zinakhalaso bwanji kiti nkhaniyi ikakhale kwa bwana Kenyatta. Bwanawa ndiokaikitsa machitidwe awo zedi, anatigulisila zotsatila zachisankho
There no professionalism at Times group. Madalitsa Mussa and George Kasakula sensationalize issues because they want money. Bravo Chaponda
Chomvetsa chisoni ndi a Kasakula ndichakuti ndi Chaponda nde kunyumbanso madam Flora Suya anthu kumakuchindirani inu muli busy ndi propaganda..kikiki …Ine ndangodutsamo.
It is clear that Chaponda will win ndipo wina asanamizirenso judge.Amulipire.
Or upange ma tricks Dr chaponda chimanga koma nyengo ikasintha 2019 udzamangidwa basi
Chaponda will win his maizegate case and stupid Kasakula and his friends will pay him bigly.
Well done Chaponda suing Times Fools. They made everyone believe maizegate hoax
Times Group lost their integrity long time ago? What do you expect from Kasakula,Brian Banda and mnyamata wadziphuphu dzosaona nyengo uja otchedwa Madalitso Musa.This is payback time!
Kukana kuti unaba, lero bwanji?
Chaponda did well to sue the overzealous times group.Its only in malawi where people think can say or write anything they think without consequences.Ena atengelepo phunziro.
6 months yonseyi sanakomzekebe? zopusa basi! Times Group and its goofy editors can run for now but will not hide. Karma is a bitch!
Times Group is worse than MBC. Serious Journalist like Ntchindi Meki left because they can’t be mkhwapa mwa MCP.
To prevail in a defamation case you have to show malice and the absence of any substance and truth in what was written or said about Chaponda. That is a tall order but knowing our judges anything is possible!
Daily times is full of MCP Propaganda.They are no better than MBC. People who are FOOLS believe in their news without seeing the MCP element in it. Zodiak, Nation news paper and Capital Radio are the only professionals reliable to reporting news. I will not be surprised with Chaponda’s win on this one.
Chaponda will prevail in this case. Atolankhani adyerawa anakomedwa ndi nkhaniyi because they thought Chaponda would silence them with money.Well done Hon. George Chaponda.Lets meet in court
You may hide the truth in the flames that engulfed your office, but you know the truth. Sometimes those in power think they are so powerful that they can hide the truth and threaten those who seek to reveal, but the truth is the truth no matter how deep we want to bury it, one day it will out
Chaponda anaonongeledwa mbiri ndi akanganya amenewa.Amulipire kumene.
Chaponda will win all these cases. Times avoids reporting whenever court proceedings are his favour.
Kangaaroo tricks /crocodile tears
from dpp crooks
Calling themselves field marshalls
embezzling peoples taxes !!
THERES GOD !!
God will not punish Chaponda or other DPP officials just because you said so. He is the only judge.
I’m not surprised that people are leaving Times Group.You luck objectivity.
mbamva izi …za DPP
Times Groups imaonjeza! Bravo Chaponda
Anaputa olakwika! lawyer from Yale University