China ‘commodity aid’ for Malawi: Donate Police vehicles
Malawi Police will receive motor vehicles donated by the Chinese government in the form of commodity aid, Finance Minister Goodall Gondwe told parliament on Friday.
The country is grappling with increased cases of armed robberies and recently official from the Embassy of the People’s Republic of China s warned that Chinese investors may decide to relocate to neighbouring countries due to insecurity in the country.
China has decided to empower Malawi Police in cracking down on a recent surge in violent crime in the country.
Gondwe said the Chinese commodity aid is worth K2.3billion (about US$5 million) in form of vehicles.
“This will be additional to some 50 vehicles procured by the government [of Malawi] during the year and will go very far in relieving government of the need to procure more vehicles for police in the 2015/16 financial year,” said Gondwe in his Budget statement.
Gondwe said it is “crucial” that Malawi should start restructuring its fiscal framework without expecting budgetary support.
Follow and Subscribe Nyasa TV :
Pakatha chaka chimodzi muzizati ndalama zina Tagura magalimoto ku CHINA..ngati mwachitira ndi stadium(Bingu national stadium) munabwera koyamba munati achina atithandiza ndi stadium,kachiwiri munasitha muli ndi ngongore ya 20b tizibweza pang’onopang’ono for 20years amanga mastadium awiri pano nde mukuti ndalama zomwe zapita ku Sports pa budget akufuna amalizile stadium(Bingu national stadium,chenicheni ndi chiti?mukangopanganso ndimangalimotowa Tizamacha!!komanso kodi Galimoto imeneyi mukuti kukhazikisa chitetezo kodi ndi nkhondo kapena chani?mukufuna muzitipha tikamakuzuzulani ndi ziwonesero?
Inu Matchalenizi Nanga Chimanga Simugawa? Chaka Chino Kulibe Chakudya Chokwanira
basi kusangalala kumakambilana za donation.pangani za malipilo a wanthu,amalawi anakakhala mankhwala bola magalimoto,mumalephela kuthamangitsa mbala nkumati mulibe fuel,kapena izo ndizoyendela mikozo
Can’t you pls donate us with mabomba atimkenawo?,cox kumalawi kuno nde zafika pa worse tsopano,kuyambira zachuma,zamaufulu,zandale nde nanji!,mabombawo mwina akanatithandiza kupanga restore dziko lino,ndakwiya nanu nanu atsogoleri adwera inu!,stuped zanu!!
Thanks 4 the gift,i hope everything will endup well,coz MW is the peace country….
THE VEHICLE ON THE PICTURE IS JUST A SAMPLE AND BELONGS TO MALAWI POLICE. ITS NOT ONE OF THE VEHICLES FROM CHINA. THE CHINESE CONSIGNMENT IS YET TO ARRIVA IN THE COUNTRY. UMBULI BASI!
OTHER SO CALLED DONORS MUST EMULATE THE CHINESE! DONT YOU SEE WHAT CHINA IS DOING.
Mtipatsekoso mifit ndi ma bomba. Bola osadzatikumba…….
Point of correction,
China sichimachita donate, TIZAPEREKA NDALAMA NDITHU, NDI NGONGOLE IYI.
Malawian we must obey chinese government for helping to archive development in a country,koma sitimva kuti aba magalimoto azikanyamulira zokolora