Email a copy of 'Immigration offices for Eastern Region ready for commissioning in Mangochi' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Immigration offices for Eastern Region ready for commissioning in Mangochi' to a friend
Malawi Congress Party (MCP) president Lazarus Chakwera on Wednesday welcomed Karonga-based fearless activist Steven Simsokwe to the rank and file...
A immigration, chonde help kupanga deport this guy working for Jhpiego, he is a Chief of Party at Blantyre Keza House. This guy is torturing Malawian workers, he can just work up and decide who to fire, change policies akangoganiza, kuzikundikila zinthu. We are living in fear at Office coz u can’t speak ur views u r gone. He is from Burundi, wamtali, wakuda. Anyone below him is useless…. Very soon tizamugenda watikwana. His boss ku LL Country Director ndi worse, pliz pliz apezeleni zifukwa azipita kwawo atikwana shaaaa.
Haah!! I support u…Kafukufuku the analysis achitikepo pamenepa basi. Ameneyu mumuuze kuti azakwela ndege yozila ndi dothi la kumadambo akunkhami. Foreigner wa dziko lina kkkkkkk azipanga zosantabwa kuno? Komanso a Jhpiego kupeleka mipando yonona yokhayokha kwa anthu obwela bwanji?
Wawa Medi kumeneko ndiye timati kubwela ukuyitha
Really, nothing can be done until the country introduces the Social security system!!!!