Email a copy of 'Malawi airport police intercepts Ukraine bound Cannabis' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Malawi airport police intercepts Ukraine bound Cannabis' to a friend
Cash-rich and powerful Minister of Local government and rural development, Kondwani Nankhumwa has said he will make a K3.5 million...
Guyz, Ananyamula chamba chanj anthuwo kod?? Reggae kapena kwasakwasa??
munthu akadya kuti abale tamusiyeni ma business akuvuta ndalama aitenga kuti munthu.mukomeleni mtima nzanu abale adyeko. sichina chimawapangitsa anthuwa ndi umphawi. alaekeni akagulitse bwezelani lupanga mchimake
chamba ndi ndalama, si bomba la nuclear ai. Tiyeni tiwalore amalawi ayambe kulima chamba…….akakhala awo amasuta chamba ndikhalidwe lawo simungawaletse…..amasuta in private.,,,,,, koma chamba ndichabwino kupangira zinthu.