Email a copy of '21 Malawi army soldiers face military court over misconduct in DRC' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

18 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
Innoxy
Innoxy
5 years ago

Malawi isiye kulimbirana nyanja ndi TANZANIA chifukwa DZIKO la TANZANIA lili ndi ASILIKALI pomwe ife tilibe.Choncho tingaonongetse ndi kuphetsa anthu osalakwa mziko muno.Kumangodya nyemba ku barracks ndi kuononga ndalama zaboma for nothing ku nkhondo ndi kumathawa, inu mungasiye mifuti ndikumakaonera mpira kuli kuthawa??.ASILIKALI Aukape.

Innoxy
Innoxy
5 years ago

Dziko la malawi lilibe asilikali, adzatipha kuno asilikali amaiko ena poti ku malawi kulibe asilikali.Kunkhondo mpakana kusiya zida ndikumakaonera mpira zoona agalu inu?.

mjiba
mjiba
5 years ago

Vuto ndilakuti kutumiza ku mission chifukwa choti pali ndalama pamachuluka kukondela. Amapita kumeneku ndi anthu oti usilikari weniweni mulibemo koma ziphuphu zopasa mabwana. Muzawona kuti ma khuki, ana ongolowa kumene ngati ali ana amabwana kapena azibale awo. Ndi ena amene sangakwanise ntchito yaku DRC ndi amene amasankhidwa chifukwa cha ziphuphu. Izi sizodabwisa.

Zambulo
Zambulo
5 years ago

Very disgusting and embarrassing news. Apa the whole world knows kuti ma soldiers aku Malawi amathawa nkhondo mpaka kusiya mfuti. Mukalembere ntchito yakolopa mzikumba popeza kutchire kwakulakani. Mumangodziwa kuvina perete basi

Payoniya
5 years ago

Mbuzi za anthu…Ndendimuone wina Ali fwefwe Ku ViBES lero..Ntchito mahule ndi kuba mafuta agalimoto basi. Nanga TATa iziyendera neutral…MT Zomba airbase ndiyamba kukutchulani..

Angoni apaphata
Angoni apaphata
5 years ago

Timadabwatu ife akamati mdf is a disciplined army kuti koma akunamiza ndani kwenikweni. Kudzikwata ndi chala. Idzi ndi dzidakwa basi mowa wakenso wopemphera makani

BigMan
BigMan
5 years ago

No comment.

Atate
Atate
5 years ago

Abweze mfuti zomwe anasowetsazo tikuzifuna. Zoona msilikali kuthawa ngati galu okuba ndiwo mu mphika kwinaku atapanira mchira. Shaaaaa.

Achiswe.
5 years ago

This looks like a grave breech of discipline, if not actual cowardice. The MDF are so ‘brave’ when dealing with their own citizens at home in Malawi, but appear to lack courage when facing a real enemy.

ananveruwa aku veterinary ukoo nsewu wa midima
ananveruwa aku veterinary ukoo nsewu wa midima
5 years ago

Sopano amathawa chani mayesa analumbira ndipo timawalipira ma Allowances a misonkhoyathu on top of their UN dues zachibwana eti mwatipangisa manyazi zitsiru za ma soldiers anzanu analolera kutaya miyoyo yawo kuzipereka koma inu mumaganizira kunyenga achakazanu kunoko ku malawi alaaaaaaa mulandire displine basi komaso nanu ma coporal aku MDF muli ndi vuto ndi ziphuphu mumatumiza anthu opanda siliyasi pa ntchito anthu ozipereka mumawasiya coz simudyanawo bwino osawalemba ntchito kumalemba mbuzi zawanthu nanga look now look zachibwanatu izi aaaaaaa

Read previous post:
Meke recalls veteran strikers in Malawi squad to face e-Swatini

Malawi national football team caretaker coach Meke Mwase has named his final 20-member squad for Saturday’s 2020 Championship of African...

Close