Malawians loot Burundian owned shops in Kasungu: Police station torched at Nkhamenya
Malawi Police fired teargas in in Kasungu to disperse some Malawians who were baying for the blood of a Burundian whose dog has killed a child.
The five-year girl was bitten to death by the dog Monday night at Mtambalala village.
In anger, some Malawians have taken the law in their hands, looting, destroying and setting on fire shops of Burundian nationals.
The people claim the dogs ate part of the body of the girl.
Still in Kasungu, there are running battles at Nkhamenya trading centre as police are battling vendors who want to kill a suspected habitual criminal in the area.
The trading centre was designated a no go zone as the vendors turned violent.
A police station and cars have been torched by the angry mob.
Follow and Subscribe Nyasa TV :
Is there still war in Burundi? Why can’t these people go back to their country?
In which world do you live in? Haven’t you heard foreign investors before?
Amalawi osamalowesa ndale pazilizonse kumasata khani adpp zikuonesa kuti mcp inawinadi mukudana nayo kwambiri samalani
ndi mbava yanu mr Tippex purofesa wakuba munthalika
Iwe mjiba mwina zikanakhalabwino kuti mwana waphedwa ndikudyedwa ndi galu wamu Burundi akanakhalawako ngati umabeleka. Apolisi chimene chimawavutanso ndikuthamangila kuthila utsi anthu pamene zinthu zaonongeka aone kuti angathese bwanji vutolo iwo busy fefefe utsi zomwe zimaonjezelanso mkwiyo😢😢😕
Alendo a ku South, a Lhomwe, Klima fodya
Musati Malawians ngati mutu wa nkhani. Mutu wankhani ndi anthu osatila chipani cha MCP awotcha Police ndi kuphwanya manyumba a ma Burundi.chipani cha nkhanza chayamba kuwonesa mchitidwe wake woyipa wodana ndi Police kudana ndi anthu obwera zonsezi pansi pa utsogoleri wa mbusa Chakwera ndi a Chimwendo kalanga ife tikulira nthawi ya baba a Tembo kudalibe zimenezi tuwona lerozi MCP kumawotcha ndi kupha Ma Police
Mbuli iwe! Zokupha mwana zikukhudzana bwanji ndi chipani? Zokhudzana ndi chipani ndi zakuti alomwe nonse tikuthamangitsani ku central ndi ku North. Muzipita kwanu ku Thyolo ndi Mulanje!
Which issue are u commenting you Simao Siwedi? Is there any mention of MCP in the story? People were angry because the burundian could not take care of his dog. This could be done even to lomwes when something goes wrong. If daughter or your relative is bittern to death by the dog , would you remain quiet? So be objective when commenting.The isse is to do nothing with MCP
Apa vonse vopempha nawo minda ku kasungu are now very scared because imagine if all minda yobwereka ija were to be taken back. Nawo awa ma bulundi achulukitcha i.e they are all over Kasungu villages kulima nyemba etc.Minda vene vake(vinyau sivi sewera paja) vikulandani tere.
Tetere apa vinthu vose visintha. Nanga Vobwera vose vili chaje lulya mmiji yose ngati mayiwawe.
Chakwela bloodshed spirit in action. Please help us God remove this spirit. Chakwela has denied you.
sizikukhudzana
Iwe ukuti chakwera bloodshed mwana wajibwa ndi galu wa Mu Burundi Uyu anatumidwa ndi chakwera or wakwanu pitala odya ma albino undisamale sadziwa kuwawa kwa Imfa Ya mwana osalakwa
This lawless Ness was not there.Ask ABUSA Chakwera for authorising blood sheding Mtambo for for disregarding court proceedings and CHILIMA for teaching youngsters to disrespect and be impudent to the elders and old and to be unruly.
There is no leader in this country. Things have totally fallen apart.