Malawians loot Burundian owned shops in Kasungu: Police station torched at Nkhamenya

Malawi Police fired teargas in in Kasungu to disperse some Malawians who were  baying for the blood of a Burundian whose dog has killed a child.

The irate vendors have burnt down Nkhamenya police station and three vehicles in the violence.

The five-year girl was bitten to death by the dog Monday night at Mtambalala village.

In anger, some Malawians have taken the law in their hands, looting, destroying and setting on fire shops of Burundian nationals.

The people claim the dogs ate part of the body of the girl.

Still in Kasungu, there are running battles at Nkhamenya trading centre as police are battling vendors who want to kill a suspected habitual criminal in the area.

The trading centre was designated a no go zone as the vendors turned violent.

A police station and cars have been torched by the angry mob.

Follow and Subscribe Nyasa TV :
Follow us in Twitter

29 replies on “Malawians loot Burundian owned shops in Kasungu: Police station torched at Nkhamenya”

  1. Amalawi osamalowesa ndale pazilizonse kumasata khani adpp zikuonesa kuti mcp inawinadi mukudana nayo kwambiri samalani
    ndi mbava yanu mr Tippex purofesa wakuba munthalika

  2. Iwe mjiba mwina zikanakhalabwino kuti mwana waphedwa ndikudyedwa ndi galu wamu Burundi akanakhalawako ngati umabeleka. Apolisi chimene chimawavutanso ndikuthamangila kuthila utsi anthu pamene zinthu zaonongeka aone kuti angathese bwanji vutolo iwo busy fefefe utsi zomwe zimaonjezelanso mkwiyo😢😢😕

  3. Musati Malawians ngati mutu wa nkhani. Mutu wankhani ndi anthu osatila chipani cha MCP awotcha Police ndi kuphwanya manyumba a ma Burundi.chipani cha nkhanza chayamba kuwonesa mchitidwe wake woyipa wodana ndi Police kudana ndi anthu obwera zonsezi pansi pa utsogoleri wa mbusa Chakwera ndi a Chimwendo kalanga ife tikulira nthawi ya baba a Tembo kudalibe zimenezi tuwona lerozi MCP kumawotcha ndi kupha Ma Police

    1. Mbuli iwe! Zokupha mwana zikukhudzana bwanji ndi chipani? Zokhudzana ndi chipani ndi zakuti alomwe nonse tikuthamangitsani ku central ndi ku North. Muzipita kwanu ku Thyolo ndi Mulanje!

  4. Which issue are u commenting you Simao Siwedi? Is there any mention of MCP in the story? People were angry because the burundian could not take care of his dog. This could be done even to lomwes when something goes wrong. If daughter or your relative is bittern to death by the dog , would you remain quiet? So be objective when commenting.The isse is to do nothing with MCP

  5. Apa vonse vopempha nawo minda ku kasungu are now very scared because imagine if all minda yobwereka ija were to be taken back. Nawo awa ma bulundi achulukitcha i.e they are all over Kasungu villages kulima nyemba etc.Minda vene vake(vinyau sivi sewera paja) vikulandani tere.

    Tetere apa vinthu vose visintha. Nanga Vobwera vose vili chaje lulya mmiji yose ngati mayiwawe.

  6. Chakwela bloodshed spirit in action. Please help us God remove this spirit. Chakwela has denied you.

    1. Iwe ukuti chakwera bloodshed mwana wajibwa ndi galu wa Mu Burundi Uyu anatumidwa ndi chakwera or wakwanu pitala odya ma albino undisamale sadziwa kuwawa kwa Imfa Ya mwana osalakwa

  7. This lawless Ness was not there.Ask ABUSA Chakwera for authorising blood sheding Mtambo for for disregarding court proceedings and CHILIMA for teaching youngsters to disrespect and be impudent to the elders and old and to be unruly.

  8. That life is bad, Malawians ur stupid in Nkhamenya change that life,a rest them for life it will be better,Africa is one

    1. Obviously you are too dull to understand human behavior when there is no leadership or they don’t recognize the leadership available. I know that there are some foolish people who are saying that leave these central people destroy their region. That’s what Muluzi did. He thought by destroying agricultural establishments in the central he will destroy MCP and chewa not knowing that he was destroying the country’s money maker. Now you find his tribal mates being butchered in xenophobic RSA because he destroyed their jobs and the industry that sustained their small scale businesses. Foolishness abounds indeed in the south.

      1. This is what we call POSITIVE THINKING. People seem not to understand what is really happening. This country has always had emergency presidents since the fall of Kamuzu in 1994 and these are the fruits that we are reaping. This is just the beginning and a lot is on the way. Just wait.

      2. TRUE TRUE TRUE.CENTRAL REGION MONEY MAKER.ANY LEADER WHO THINK CAN DEVELOP MALAWI MINUS CENTRAL REGION FARMERS WALEMBA MMADZI.VUTO NDILIMENELI.WAKEUP.

      3. A malawi dziwani ichi akaunjika mumagulitsawo popanda alimi palibe business.Kumbukani kale ulimi ukuyendabwino chamama wimbe madisi inali misika ikulu ikulu anthu amachoka ku lunzu ndi mabelo kukathela kuchamama komwe pano alimi ndi osauka.Dzutsani ulimi alimi akhale ndi ndalama mavend a akhala ndi ndalama ndipo azikwera galimoto yawo pokagulitsa osati uncivilized thinking yopha ulimi chigawo cha pakati.Lero njala chaka ndi chaka mdziko.koma nthawi ifika pamene anthu osankhidwa ndi mulungu atsogolera mtundu wa a malawi ulimi udzuka.alimi adzakhala ndi ndalama mavenda adzakhalanso ndi ndalama za alimi omwe mukuwanyoza lerowa ndiye tsogolo lanu la buzinesi komanso tsogolo la dziko.A malawi ino ndi thawi youzana chilungamo chifukwa lero akulira ndi aliyense Venda ndi mlimi yemwe.Chotsani kuvala mmtundu kapena chigawo poganiza.Ine ndimaneneratu kuti olo atakhala ntsogoleri wa chigawo changa kaya mtundu chitsiru ndi chitsiru.

    2. Benjamin, war in your country is over. You have overstayed, please go back home in Burundi. We are not stupid.

      1. Malawianas are always trekking to South Africa why??? Do we have a war here??? Palibe dziko limene kulibe ma foreigners ngati ndikunama please tell me.

    1. That is if you know kuti Nkhamenya is full of Lomwes kudzalima mmimndamu, your comment would have just be neutral to avoid being called stupid.

Comments are closed.