Email a copy of 'Minister probes Kasungu hospital for rejecting  free blood donation due to lack of allowances' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

10 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
thako lambeta
thako lambeta
7 years ago

This job is not a calling these people were employed and they deserve ma allowance pa zinthu ngati izi ikankhala caling bwenzi kukukhala ma interviews? Bleeding a hundred pple its not a joke that meant kuyitana anthu oti ali pa off kuzagwira vep for nothing is that fair?
Iwe kumpalume tikuthamangitsa palibe za yes apap.

Mapuyamurupare
Mapuyamurupare
7 years ago

Bwana Kumpalume kwina kulikonse otolere magazi amalandira allowance.
Ku Kasungunso ayenera kuasidwa ma allowance basi.
Bwanji a Phungu aku nyumba ya malamulo amalandira ma allowance
atango nkhala pa mpando ku perliament inu zimenezo bwanji simumawa fufuza.

Achipatala nonse musiye kungwira ntchito mpakana apepetse pa nkhani imeneyi kuti zinthu ziziku yenderani.
Panopa achipatala musamale anthu azikutolani ngati simugwiriza. Ngati zimene zili ku UNIMA podedera College of Medicine Lecturers.

ellias
ellias
7 years ago
Reply to  Mapuyamurupare

@ Mapuya Murupar…chifukwa sukudwala nkona wayankhula choncho. Asiye kugwira ntchito cos of allowances? Agwire koma not full day. Ena ALI PA OXYGEN, ENA PA MA DRIP NDE UKUFUNA KUNENA KUTI THEY SHUD ABANDON THEM? udzadwala

PITA MZIPATALA ZA BOMA AND SEE HOW PREGNANT WOMEN ARE BEING TREATED, BEING CALLED ALL SORTS OF NAMES BY THESE SO CALLED NURSES. Ubwino wake tili mu multiparty, tidzingowaswa akayankhula mwano like the mangochi nurse. Its only Kamuzu time when health personnel were respecting patients.

Kanjedza
Kanjedza
7 years ago

The ißsue of allowances is nothing new. It happened a couple of years ago with mulanji hospital . The nurses and the trainee nurses and other staff declined to offer their assistance for free medical camp -doctors were coming from uk. Finally the camp was moved to the mission hospital near mulanji. The seven day camp treated over 1,000 patients for eye ailments, minor surgeries,free medicines and spectacles. Every day the camp was feeding over 700 patients and their attendees. Thanks to everyone at the mission hospital . They did not ask for even one tambala. Shameful by mulanji hospital… Read more »

JJ
JJ
7 years ago

donating blood on a Sunday when possibly the staff were off to church? Why did you not go on Saturday? kuopa kuphwanya Sabata, and its OK with other christian faithfuls who pray on Sunday. And again, 100 donors? That is no simple job. Next time make flexible arrangements for the hospital staff- Pitani mkati mwa Sabata

Kanjedza
Kanjedza
7 years ago
Reply to  JJ

When you are doing good service in the name of humanity, the lord will forgive you for not coming to church on sunday.

che mangochi
che mangochi
7 years ago
Reply to  JJ

Iwe mfiti anthu akuchipatala ndinu afiti nonse

amoyo salekana
amoyo salekana
7 years ago

kumpalume are u serious on this or u are saying out of emotions. nthawi inapita imene anthu akangot Yes bwana, mumafuna munthu achite attend The whole 100 people on odd hours without allowance. iwe ukayenda ndiye upasidwe ma allowance.

Ndipo ukangoyesa kuchosa Swap uwona, ukachiza wekha abale ako. love ur health workers

soon there will be no angels on earth

kusungu chirwa
7 years ago

This is bad for the “KUSUNGU” hospital as per the picture above.Playing Politics with peoples’ lives i presume.

James
James
7 years ago

Muchita check ma conflict of interest links between Dr Moses ku Central medical stores, and Malawi pharmacies amalandla ma contract mu billions.. Alipo sharholer mu Malawi pharmacies

Read previous post:
MCP mourns a member who died Sunday in road accident

Opposition Malawi Congress Party (MCP) is mourning a member of the party who died in a car accident after he...

Close