Email a copy of 'Peoples Party still too broke for convention' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Peoples Party still too broke for convention' to a friend
It was all smiles for a 20 year old Dennis Mkonongo this week when workers working for Zhejiang communication construction...
Koma dziko la pansi ayayaya. These are the people that were flying on moneys. I can not understand. Now they are saying they are broke. Kkkkk we should stop praying with the world
Just merge with MCP
AAAAAAAAh zosamveka. Chilipo nkhani sindalama. Mukubisalira kundalama. Chibwelereni amai akhala akupanga so many campaign rallies live on zodiak and ufulu radios. Ngati ndizoona kuti ndalama zakuthelani ndibwino musapikisane nao. Amalawi tatopa ndi kubeledwa ndalama. Pakhale lamulo lokhazikitsa mulingo wandalama zoti chipani chidzikhala nazo monga muja achitira mabanki. Onse osafikira pa mulingo umenewo asamaime pachisankho. Mwina korapushion itha kuchepa. Umphawi wamzipani ndi umune ukukolezera korapushoni. Pano zipani ziribize kudobadoba amwenye ndi abizinisi kuti apeze ndalama. Akalowa m’bomamo choyambilira ndikubweza ndalamazo. Nawabizinesi akapeleka ndalama amayembekezera phindu. Choncho PP MUNGACHITE BWINO KUNGOKHALA PANSI. ZAVUTA BASI. MASINTHA IDAULURA ZONSE KUTI MPIKISANOWU MWACHEPA NAO.
Waiwerenge Joy wadzindikira kuti sangawine bola za cashgate zakezo angosunga adzidya yekha
Stupid. All the four years we were able to follow you spalishing money in a foreign country and today you have the guts to say you have no money to hold a convention while a smaller party like Aford can be able to hold one.
Hahahaha Malawi is a playground