Email a copy of 'Police nab two men for smuggling Malawi Hemp to Mozambique' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Police nab two men for smuggling Malawi Hemp to Mozambique' to a friend
Be Forward Wanderers veteran midfielder Josephy 'Shakira' Kamwendo will join Tshakhuma Tsha Madzivhandila FC , a South African First Divison Side...
nde zachambazo!!! mwasowa chochita migwanya inu eti??? kodi magulu amene mukuyenela kuwatapa simukuwawona??
Tangowasiyani anthu awa akanatibweretsera forex. Osapita kukagwira awa akukhapa ma albino bwanji?
Mbava zonse including him Will be happy if alarfat wins chisankho plus anthu a ku mpoto
Asiyeni awo. They were exporting. They’d have earned forex for Malawi.
Now chamba chimenecho agawana mabwana a police nkuchigulitsa m’Malawi mom’muno. That’s the sad truth about this whole thing.
DEAL WITH ALBINO KILLER’S —DEAL WITH CASH GATERS —NOT THIS BONYA Aaaaaa !!
Mwalankhula bwino apa
Marijuana is becoming legal all around the world but our sleepy govt is penalizing someone for selling it abroad.
Asiyeni anawo
Osadanda Arafat Hamdan a.k.a. Saulos Chilima akazangotenga Boma muzatuluka. The VEEP has ur back guys. For now he will storm Dedza Police to force Police Officers there to arrest him on your behalf.
Tsoka likalimba.
Kodi awa ndiye sakawaombola? mmesa ati akayambisa kulima chamba ku KK. Koma anthu ena?