Email a copy of 'Police take UTM’s Kalindo to Zomba: MP charged of 'insulting the president'' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Police take UTM’s Kalindo to Zomba: MP charged of 'insulting the president'' to a friend
Malawi’s music kingpin Lucius Banda has released a new single entitled ‘Moyo wa Msilikali’ in honour of Six Malawian soldiers...
One tonne of bricks.
Join the discussion…kadyankena.kalindo apa zavuta basi .
PALIBE NKHANI APA !!
Ukamazitengera zinthu pa mgong’ono matero ake amakhala ngati amenewa, ambiri mwaife tikufunisitsa zinthu zitasintha koma chikufunika ndikudikira tsiku lovota basi. Zipani zonse zikuyenera kupanga campaign yabwino, yosatodzana chikufunika ndi kutipasa fundo zoti ife tikopeke mpaka tikavotere yemwe ali ndi kuthekera kosintha zinthu basi.
Amayesa akupanga drama this is the arm of law.
Just because of his arrest I’m voting for UTM
Has Kalindo committed a criminal case? I do not support UTM but why all this? b careful !!
Athawanso bill ya K3500.00 ya Mangina ku Sportsman Bar ku Blantyre. He always promise the place by either buying one bottle of Coke just to watch a football match. He is too noisy.
Kukakhala ku Machinjriku wasiya ma bills a rent ku Area 7, 6 and Kwate. The guy is a rat Big time.
OSAMPASA BAIL AMENEYO, NDALE ZONYOZANA SITIKUZIFUNA
The arrest is not political. Hon. Kalindo just happened to have violated the Laws of the Land. Hon. Kalindo, should have known better, as a Parliamentarian.
So, no tears for Hon. Kalindo.
Pathetic… thats why serious pipo do not comment here… it appears macadet ndi mbuli zopanda nzeru comment zinthu zopusa. You impersonate innocent people. This is a forum for frustrated persons. Now, in all fairness masiku ano simasiku omamanga anthu panthani zopusa ngati zimenezo… kulankhula! really? And Mutharika Ziboda is such a good man, how can he let that to happen… ndiye kuti simukudziwa kuti even if Winiko is charged or prosecuted or killed, you are only making him a hero from zero. Nkhondo akuiputayi Mutharika ungochepetsera masiku a moyo wache… alomwe anzakewa akulimbana nawowa ndi abale ake…. ammaliza!