Email a copy of 'UTM members in South Africa on massive fundraising drive' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'UTM members in South Africa on massive fundraising drive' to a friend
One of Malawi’s top mobile phone service providers, Airtel Malawi Limited says it has so far spent K24 million on...
He Guys – Attn Mr Humphrey Mhango, wud you pliz furnish us with the directions of the venue so we can join the UTM party pliz!
And wud you pliz contact me. I am a UTM die hard but did not know that we have a grouping here in Jozi. My cel no is 0788557604, whatsapp – 0651809091. Thanks guys and keep it up!
Eshhh koma khope ndikuziwona pa zithunzipa abale. Malova okha okha. Kaya ndalamazo zikafika zokwanira kumudziko kaya? Eshhh
Kkkkkkkkkk musters abale komanso Maudindowo apatsirana kuti? Koma keep it up guys UTM is the hope for Malawians.
These are just opportunist. I know all these guys. They have failed here in SA now are aiming for a recognition back home with an aim of getting opportunities, Anyway fumbi ndiwe mwini
Makonda makonda osanyozerana atsogoleri kapena zipani.. Moyo wopusa umenewo. Aliyense assnkhe chimene wakonda. After onse mukulemba apa simungayime pa msokhano nkuyankhula.
Its far better off to raise party funds through such innovative operations. It only signifies that its the grassroots that own the party which is in complete contrast with others parties. I would like therefore to suggest that other parties should emulate this strategy and shift from the current practice where party members expect to receive hand out from their respective parties or a party sourcing resources through corrupt means. Keep It up UTM by doing things differently.
Wamva kuwawa
Mbuli izi sizikudziwa zisiyeni
Fundraising? yachani? Dziko lake lomwe mukukhalalo osati Malawi kagwereni uko ndi Zilima wanuyo
kkkkkkkkk koma abale chipani choyamba ndikupemphetsa kuti chizalowe m’boma chidzatipatsa umphawi wa zaoneni. Bola mukudziwa kuti ndalama mukusonkha panopazo ndi no return. komanso ikamazati november chaka chamawa chilima adzakhala ataiwalika ngati ma vice president onse a matukutuku a mbuyomu. By the way nyasatimes, this is the real pathfinder with a small latter (p) not a capital latter (P). I have changed my name to this one because there’s some asshole who is using my name to help campaigning his broke party and leader. Look i am in DPP with all my heart, unless you give me a valid reason why… Read more »
Sitikufuna Luna ndalama muboma that’s why tikupanga fundraise if it makes sense to you
Mumumva kuwawa UTM led by SKC
Ngati wathu uli moto wamapesi ndiye kuti kwanuko ndi phulusa lokhalokha lopanda moto pagonanso agalu
GOOD DEVELOPMENT
The Burning Up of NICO house wina alira,asowa kotapa,muyisova,ine toto