Chilima promises improved service delivery and ODL for Chileka
State Vice President who is also president of the United Transformation Movement (UTM), Saulos Chilima has said it a pity that Chileka area in Blantyre continues to wallow in pathetic services of water, health and electricity despite being the production area of such services.
Follow and Subscribe Nyasa TV :
Anthu akadzayamba kuululana ndiye kuti amabera limodzi kungoti apondetsana thats why one just rush to spill the beans. So Chilima dont cheat malawians you too is a thief thats why u wanted to steal DPP in day broad light by kayikitsa nkhope yako pa nsalu ya DPP and write Chilima 2019 Boma before convention has determined a torch bearer. Anakutulukira msanga tambwali wankulu ndiwe!!!!
KUGANIZA MWA UMBULI UKU KKKKKKKKKKKKKKKKKK SHAME!!!!!!
Chileka and all other areas indeed deserve to have those service bwana, koma inu ndi mbava munawasankhira anthu zija zatiwonongera chitukuko.
ben phili k900 million kkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkk
he is a joke
misonkhano ya chilima eyadi imachuluka ndi acinyamata, same misonkhano ya pitala kumaculuka anthu okalamba, nanga ana akamvanji kwa pitala avanji? apitapita ku misonkhano ya pitala koma zokamba zake sakuuva kanthu. only world they have grabbed ndi ili OLIMBANA NDIINE NDIZAMUNYENYANYENYA. basitu. khaye akaonesa ukali nde zero siziveka zinenea iye. mxiiiii. ndi demol;asetu iyi asiyeni aliyese amabwera ndi ndondomeko. kodi ndondomeko zinayala pitala zija cacitikapo cooneka ndi citi. angoti bwaibwai pano as may is approaching. so nkula sinabwere ku cileka nvetsani wakamba za madzi zoona ku chileka ndi kouma kovuta madzi kwa inu simukudziwa dziwani. magetsi omwe alipo amaika ndi ma… Read more »
Chilima usamaname choncho please. Mwalephera limodzi ndi gogo chalo Alamu Pumbwa Mwakalamba whose agemates Aretha Franklin, Kofi Annan and today John McCain have died. Alamu Pumbwa Mwakalamba azilondola anzawo amenewa ngakhale akuba.
go go go SAULO.
ku chileka kukangoziwika ndi dumbo lemani. no citukuko dela limeneli
ndi nyengo ira ku ngumbe/nkhumbe kumene kumacitika zoopsa. women of from different poverty levels kuzadya nyama ,ma fanta, staying at that place for days with no productive gain than kudzaona blantyre basi. DAUSI!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!
pano tikufuna zithe zovinila misonkhano. waste of time komaso kacilombo kumeneku. too much promiscuity
Musasinthe nkhani ya quota system don’t take Malawians for granted uli mmboma mono why you don’t act now?Nonsenu ndi mbava pano mukuwululana tiwonana pa 21 may ambuye akalola.
Listen to understand not only to answer His excellency was saying Chileka is nearer to the power stations
The guy has the correct message for the people. But he has not tackled land issue which has landed Wandale into a mental hospital. Your remarks at Njamba touched on the cause of John Chilembwe’s death. You’re the first Malawian on a political podium to shoot straight from the hip now make a follow-up No false starts all Malawians look to you the staff is in your hand break the rock we need water
Looks presidential