Kasambara back in prison on remand
Former Minister of Justice and Constitutional Affairs Raph Kasambara has returned to prison after being discharged by Blantyre Adventist Hospital (BAH), and is being kept on remand for alleged conspiracy to commit a crime in the attempted murder of Paul Mphwiyo.

High Court Judge Michael Mtambo revoked bail conditions for Kasambara over alleged infringement of the judge’s private space by secretly accessing private information.
In the case, Macdonald Kumwembe and Pika Manondo are facing charges of conspiracy and attempting to murder former Ministry of Finance budget director Paul Mphwiyo at the gate of his Area 43 house in Lilongwe on September 13 2013 while Kasambara faces the charge of conspiracy to commit the crime.
Kasambara has been at hospital for heart condition but according to BAH sister-in-charge, Magret Takomana, he was discharged on Thursday.
Commissioner of Prisons Kennedy Nkhoma said Kasambara was remanded at Chichiri Prison after being discharged. He was reportedly taken to Zomba Maximum Security Prison later.
eeh koma nde anthu mukutokotatu mavuto a kasambara ndi anu musiyeni asova yekha inu wonanu mavuto anu
Tikudikira chigamulo
Chitani kuti a Mw akukhululupireni ndikukhala ndiyembekezo mwa inu. Coz ndikutheka ena alipo amayenera kukhala naye limodzi mkuluyi ku ndende
Ife nkhani ndi Maggie…iiiih mwana kazi anabadwa uja yayayaya
@Tuyuni…Mtambo is from Zomba. He is not from the North. So is Kachale.
A Raffu, k0ma ife timkadziwa, Us0va Maravi wats0pa,,,,,,,,,, U iz a Pr0bem, mei be sumadsiwa,,,,,,,,,
Jjji
Ku Malawi tichita nkhondo posachedwapa tiona!
Amangidwe basi.
Palibe kuchitira mwina akagwire ntchito yakalavula gaga kwa zaka khumi ndi miyezi isanu ndi umozi
We want judgement not remand. Minus Kasambala we have only one lawyer inakawi who is Wapona Kita.Will he manage alone?
Ralph naye awone zokhoma,
Wakumana ndi mitu imzake amazitenga dolo kwambiri ameneyu
Iiii mumvereni chisoni. Kwasala tchiretu moto umapita komweko. Mudzaziona.
wish you well let God be your guarding angel though i walk in the valley of shadow of death i fear no evil for God is my fortress he shall deliver and under his wings you shall find refuge
Mtambo…read what Tuyuni has said… Wachewa mbanthu yayi..uzamulira iwe nkhanila cchweeeeeeee
MTAMBO KACHALE KNOW THIS BIBLICAL TRUTH THE TRUE JUSTICE OF GOD NOT THE JUSTICE PURIFIED BY TRIBAL VENGEANCE SAYS. THE WAY YOU MEASURE OTHERS IS THE WAY YOU WILL BE MEASURED.
I hope this process will make Ralph mature and not behaving like a 15 year old boy commenting on serious issues on Facebook. Grow up man mynthu above 50 you still behave childishly!
The law is the law no matter who you are. Pepa Maggie mwamuna wakoyu mmmmh too much zochitika and am sure God didn’t mean you to get married to this guy…iiiiish wapilira too much.
ADA KASAMBALA MWE AVUMBWA UKONGWA
NAA IMWI
ATONGA TE VIGUMBULI LIMU ADA AA
nsena nzeru ulibe..instead of allowing justice to prevail u busy writing zako zamabodzazo..kasambara be ur brother? no one is above the law… mwaoneselatu kupanda nzeru kwanu kosetu apa…
Uyu ndiye afere konko abale amatienjeza bad a Malalwi ngati ndife zitsiru
A tuyuni pepani go & check,mtambo simchewaa,raph ndi mtonga,palibe chikumukhudza Mmwana wa mchewa apa,malamulo agwire ntchito bassi!!!
Zochitika za masiku otsiliza. Wowerengawe khala maso.
Kasambara sanabe, komanso sanaphe. Chomvutitsira nchiyani, agalu inu?
PleaseKasambala stand upright and talk to me into my eyes. Why shy? Time to test prison life. Ukhala track ya nyapala iwe. Kukankha track man.
The wages of sin is death
The hunter has become the hunted. The Falconer can not falconise. All hell has broken loose on the former best lawyer. Things have fallen apart.
Wishing You all the best Kasambala, but You justice Mtambo you are very stupid
achewa amatetezana ngakhale wina atalakwa koma iwe kukhomelera m’bale wako.achewa awo si anthu ayi, oro uwapangire chabwino sayamika tsiku lina azakusiya uzafuna abale ako. Chitsiru cha munthu Mtambo.
Nkhani yake yomwei kapena ina inu a tuyuni
Amajaila ameneyi amayesa ngati dziko la malawi ochenjela ndi iye
Watch his food, and make sure whoever brings it eats a good sample. Amwanso viagra wina kuti mtima wake uyambe kuthamanga.
It will cost his time to delay.let he be convicted and start serving.thats one time
Malawi at 51, the untouchables are going down
What about Phwiyo? When is he going to be locked and rot in jail? He is the main actor in all this.
All the best Ralph. We expect to hear the truth and see justice being done. Dont play cowardice
Chichiri prison officials has confessed that they were getting orders from DPP regional governor to have killed Ralph hence poisoned in hospital so that he should not be popular. Where is justice, mary kachale is also being by party officials, APM distanced himself by saying he doesnt infringe in judicial.
a msena ndinu munthu wochititsa manyazi, lets respect the laws. osamangobakira zilizonse…. ungamve!
Ufera konko iwe!
Sorry my. Brother Mr intelligent
Kasambara! Kasambara! Kasambara everywhere Kasambara.
Kodi Kasambara yo ndi this lizard-like-looking frog or frog-like-looking lizard?
Ine I have always thought kuti ndi munthu tu!
Next two days he will have a relapse. Just buy a good cell for yourself – with bed & matress, fridge & tv and speed up the trial mwina nkutuluka. Also stop humiliating your fellow legal practitioners. As you can see, it has landed you in an awkward situation.
adwalanso pompano ndipo azingodwala mpakana next year. if ujeni did it, why not ralph? dwalanso i say…
Ok Kasambala akufunika Makako wandikwana Mochuluka
Far reaching consequences of greed and selfishness.
From hospital bed to stinky and filthy floors of prison toilets
hehehehehehe….tiziona mmene zithere. ameneyu alangidwe ndithu
Eish from Hospital to Prison, koma dziko ndilowawa ili eti? kikkkkkkkkkkkkkkkkk!
Hope Kasambala will tell the truth while in remand
Shaaaaaa sapheka wapheka.