Malawi church says stop calling it ‘Ass of God’
Malawi Assemblies of God church has issued a memo calling for all churches to stop using the phrase ‘Ass of God’ on their signposts.





An internal memo released on 19 September and directed at the Church’s leaders, the President of the church Rev Edward Chitsonga, who signed the memo, advises that ‘Ass’ means a booty, a donkey, a fool or the rectum itself and thus was not a word the church needed to be associated with.
“Kindly inform all Pastors under your jurisdiction ro refrain from using the abbreviation on their signposts. Let us write the name of our church in full: Malawi Assemblies of God,” says the memo.
‘ Ass’ on the sign post was being used as an abbreviation for Assembly.
Lucky they never adopted ‘Asses’ as an identity for the church’s faithfuls.
Hahahahaha!
or otherwise pemphani moderator to withdrawal your comment here
A Ndyomba, ngati mulibe zokamba just keep quite. Ndi za Mulungutu izi. Don’t sin jockingly. Pamenepo mukumutukwana ndani? Lapani ngati mumadziwa kapena kumvapo za Mulungu.
Zubwera mochedwa. Nawo ma yo aku USA kusocheletsa anthu too much
Kodi azibusawa ma PHD akumawatenga kuti
Kikikiki! koma iwe Muheya, mpaka ‘Asses’ for the church’s faithful!
Matako a ambuye kkkkkk
kkkkkkkkkk hahahahahahaha aise Ndyomba its more like NYERO la MULUNGU! Iwe ukudana ndi comment ya Ndyomba matako ako. Kodi nkhaniyi walemba ndi Ndyomba? kodi mmayesa ngati Mulungu wanuyo ndi choopsezera anthu eti? Kodi mukudziwa kuti dzina looti mulungu kuno ku SA limatathauza Nzungu, kapena kuti munthu oyera khungu mchiyankhulo china? Kuti muone ndi mzungu yemweyo amene anabwetretsa baibulo kutiuza kuti kuli mulungu ndipo mulunguyo ndi oyera khungu. ndi kupanga anthu ambiri kukhala a khirisitu, ndipo a khiririsitu ndi amene ali very judgmental pano pa dziko lapansi. Ngati siukuchita zomwe akukhulupilira iwowo amati akuti ukupsa ndi moto olo ukaonongeka. koma ukachita… Read more »