Peoples Party still too broke for convention
Peoples Party (PP) say it is too broke now to hold an elective conference and could not say when exactly the convention would be held.
The party’s publicist Noah Chimpeni said the party has not even started preparations for the convention due to lack of money.
“We don’t have even the money for the preparations. However, we will still hold the convention,” he said.
Chimpeni however said all the party supporters are rallying behind the candidature of former president Joyce Banda as their presidential candidate.
Chimpeni said this has nothing to do with the decision by 13 tiny political parties to rally behind the former head of state on the 2019 presidential race.
He said there is still in conclusion on the formation of a grand coalition.
Follow and Subscribe Nyasa TV :
Koma dziko la pansi ayayaya. These are the people that were flying on moneys. I can not understand. Now they are saying they are broke. Kkkkk we should stop praying with the world
Just merge with MCP
AAAAAAAAh zosamveka. Chilipo nkhani sindalama. Mukubisalira kundalama. Chibwelereni amai akhala akupanga so many campaign rallies live on zodiak and ufulu radios. Ngati ndizoona kuti ndalama zakuthelani ndibwino musapikisane nao. Amalawi tatopa ndi kubeledwa ndalama. Pakhale lamulo lokhazikitsa mulingo wandalama zoti chipani chidzikhala nazo monga muja achitira mabanki. Onse osafikira pa mulingo umenewo asamaime pachisankho. Mwina korapushion itha kuchepa. Umphawi wamzipani ndi umune ukukolezera korapushoni. Pano zipani ziribize kudobadoba amwenye ndi abizinisi kuti apeze ndalama. Akalowa m’bomamo choyambilira ndikubweza ndalamazo. Nawabizinesi akapeleka ndalama amayembekezera phindu. Choncho PP MUNGACHITE BWINO KUNGOKHALA PANSI. ZAVUTA BASI. MASINTHA IDAULURA ZONSE KUTI MPIKISANOWU MWACHEPA NAO.
Waiwerenge Joy wadzindikira kuti sangawine bola za cashgate zakezo angosunga adzidya yekha
Stupid. All the four years we were able to follow you spalishing money in a foreign country and today you have the guts to say you have no money to hold a convention while a smaller party like Aford can be able to hold one.
Hahahaha Malawi is a playground