Phungu wa DPP ku Mangochi wati awonesesa kuti Chakwera apitilize kuyendesa Malawi

Phungu wa chipani cha Democratic Progressive Party wa dera la kumpoto m’boma la Mangochi, Benedicto Chambo, wati agwira ntchito yothandiza kuti mu 2025, President Lazarus Chakwera apitirize kulamula dziko lino.

Phunguyu lero adali nawo pa msonkhano wa chipani cha Malawi Congress umene unachitikira pa bwalo la masewero la Dzenza, ku Area 25 m’boma la Lilongwe.

Mlendo wolemekezeka pa msonkhanowu adali nduna ya maboma aang’ono a Richard Chimwendo Banda yemwenso ndi mkulu wa achinyamata mu chipani cha MCP.

Follow and Subscribe Nyasa TV :

Sharing is caring!

Follow us in Twitter
Read previous post:
Communities in Nkhata-Bay have never listened to local radios due to no signal since independence

Malawians living in some parts of Nkhata-Bay rural say they lack access to local radio stations as there have been...

Close