Protests over ‘death of healthcare system’ held in Rumphi
Hundreds of people have marched in the northern region district of Rumphi to protest against the starvation of patients in Malawi’s public hospitals.

The peaceful protestors clad in black attire, organised by the district’s civil society network, blamed government for what they called “death of healthcare system.”
The protesters were also angry at what they say is reckless public spending by government while public hospitals suffer funding.
Civil society network chairperson Eunice Banda said the protestors want President Peter Mutharika to heed the cries of patients dying of hunger and lack of ambulances across the country.
They presented their petition to Francis Puleni, acting director at the district council, who said he will hand over to the President.
Amalawi tili ndi vuto loyiwala msanga. kumbukani kuti ndalama zinabedwa za nkhaninkhani m’boma nthawi ya JB, ndalama zomwe zikanathandiza dziko lathu lino. Pano boma likuvutika kuti lipeze ndalama zoyendetsera ntchito zake. zonsezi mwaiwala kale? kusowa chithandizo cha boma ndi nkhani ya tonse ngati amalawi.sinthawi yolozana dzala.
I’m not in support of you.This is country wide agaist Peter. There is no smoke without fire.
MA FELLOW NORTHERNERS WE SHOULD NOT BLAME GOVT.TAKE EXAMPLE OF RALPH KASAMBARA WHAT DID HE DO DURING JBS ERA HE STOLE MONEY THROUGH CASGATE HOW MANY NORTHERNERS WERE INVOLVED IN THAT MASS LOOTING OF GOVT COFFERS.JUST VOTE 4 ME I WILL KILL ALL THE NORHERNERS AND BURN THEIR BELONGINGS IN THE COUNTRY.
Why is it that many CSOs and their leaders are Northerners? To say the fact these gurus have an in-built element of evil minds agaist others gvt. To hell with ur protests. You think we in LL will emulate that. Mwagwa nayo basi,
Kuba too much,,,, ine ndili ku Rumphi komkuno koma Sinddayende nawo chifukwa Kuba ndalama Zaboma ndi mabungwe kwakula, komanso kuwonjezera pamene mabungwe ambiri sakuziwa chochita, monga Ophunzitsa achinyata zinthu zosiyanisiyana M’malomwake ogwira ntchito angozilemeletsa Okha- zotsatira zake chomwe achinyamat akuziwa ndikumwa mowa ndikumakavina ku ma Birthiday paty omwe amakhla akuchitika week end iliyose m’malo osachepera 10 patsiku… Chonchi malawi ndikukhala ndimaganizo ofuna kutukuka,,,, ndizomvetsa chisoni kuti Chilichonse anthu akungoti Pulezideti ndimvula yomwe,,, Tiyeni tizikumbukira kuti azipembezo zosiya-siyana timkapemphera kuti Mulungu atipatse Nsogoleli ndiye tiyeni tikawerenge Baibulo ku mayeyu 7:7 kumatsika,, Tiyeni tikhale ndi mtima wa umunthu. Komanso tikonde Dziko lathu…….
These are the days of survival of the fittest. Days of free lunches are over. There are plenty of drugs in private hospitals.
Aganizireni anthu osauka. Empathize with them. Muganizire muli inu. These people cannot afford to pay bills at Mwayiwathu, Seventh Day Adventist or even kupita ku South Africa kapena ku India mumapita inu kuja mukadwala. Misonkho yathu ija mumadula pa salary ndi zinthu zogula ndi ku Road Traffic, ku Immigration ndi zina zimapita kuti. Someday you will pay for the suffering you are causing
MBANGE NDA NJUNGA NDA NGOMA ZILA JB WAKAMUGABIALANI NYENGO YA KAMPENI. FUMBANI KAMLEPO WAMUVWIRANI IMWE BINA RUMPHI
Sono kuvina uku si mwakhuta kale apa…vindere nadi ivi….
Bwanji osayamba kaye mwasonkhesa ufa ndikukapeleka ku chipatala kenako nkukayenda kunseu kusonyeza kuti inu nanu mbali yanu mwachita, isale ya boma??? Tikaonesesa mwinanso nonsenu apa ndi msonkho omwe simudula kupatula VAT nde muli pa fore front…Its time to be logical..tiyeni tidzuke
typical quota reasoning by Khima @24.. You want these people to dig into their pockets to cover peter’s wastage and theft of our own taxes. these people are protesting against theft by DPP and you know that
ANTHU OIPA INU, MUNADYA NDRAMA INU NOKHA, NTHAWI YA AMAYI, WHAT DO YOU REALLY WANT?
Stop relying on free food please you lazy people. What do you eat in your homes? Eat the same in the hospitals. There are many patients in our homes, what are they eating? You stupid politicians stop hiding under the issue of free hospital food.
Testing the waters thinking that this Demo would escalate to other Districts to become a national issue. It has failed the acid test.
Shameless DPP idiots on firefighting. The worst leader we have ever had as a country. You move maize from admarc thereby creating another problem. You guys are headless chickens. No wonder people call you and your president clueless. So tell me when this firefighting will stop? We may have a case very soon where the entire nation will be on fire and you and I know the end result is not pleasant. My advice, take it or leave it, please engage the opposition and other community leaders to solve some of the challenges the country is facing. I rest my case.
Boma la alomwe ili
More fire Rumphi, lest we forget mpoto leads the way! Ise saza tilije! Ma CSO a ku Rumphi tabwerani kuno ku LLs and BT muwaphunzitse anzanu kuti anthu akama manidwa chakudya ku Chipatala cha Boma timakodola!!!
Mulakho wake uti udathera ndalama????? Iweso kape eti,,,, Timaziwa kuti ambiri simumawaona anthu a chilomwe ndi diso labwino,,,, pitiliza Uwonana polekera Mbuli iwe!!!! Enanso Boma likathandiza inu muziba,,,,,,,
Achita bwino panja kuno kumalawi zinthu zili bwino anatero Mp wakulilongwe .ambuye akuoneni
Mumuuze wa DPP akumapanga ma counter demonstration tsiku lomwelo la ma demo kuti tsiku lina tizabandulana ndithu.
Do peope have right to be given free food really?
Ndalama zinathera mulakho
THESE DEMOS WERE SOPPOSED TO
BE NATION WIDE DEMOS !!!
ITS A NATIONAL ISSUE
THE WHOLE COUNTRY IS SUFFERING !!!
You are right but mbuzi za kumwera can’t see this.
patients are starving while executives are enriching themselves through cashgates
Anthu ogenga kumaliro awa, samala nawoni.
Just as Government has increased fees in government secondary schools let it swallow its pride and declare that it shall no longer provide food to in patients. Read in the paper that Bamusi was in Rumphi to persuade the CSO s not to go ahead with the march. So what happened? May be he made a low and unattractive offer or amudyela. Gaffement is serious business anatelo a Tcheya
BRAVO CSOs IN RUMPHI.. SO DPP YOU WERE WAITING FOR PROTESTS FIRST TO DONATE 100 BAGS OF MAIZE AND 20 BAGS OF BEANS. WE NEED MORE THAT IS TEMPORARY. GIVE THE HEALTH CARE SYSTEM IN ALL DISTRICTS ADEQUATE RESOURCES.
ma NGO ndinu nomwe munkapanga lobby kuti ma donars asapeleke ndalama lero mwazionatu muli pa fore frant mwati boma silikupeleka chakudya,inu osasonkhelerana bwanji kukagula matumba a chimanga kukasiya ku chipatako kuti azibale anuwo azidya????????? aliyense atengepo mbali sinthawi yomapanga ma demo iyi, kodi funding ku rumphi dho sikubwera maallocation awo akugawaa bwanji ndalama tikudabwatu mzipatalamu ati funding ikuchepa koma ma workshop ndiye week ili yonse, kodi ma allowance amenewa akuchokera kuti si ort yomweyi???? muziyamba mwapanga kauniuni musanapite ku nseu kwanuko
A day can hardly pass without our government goofing. It is an open secret and clear that this current DPP government has failed to find solutions for many numerous problems rocking the country. Instead of acknowledge failure and seek alternative views from the opposition government is busy playing fiddle politics with lives of many Malawians. It is not about the question whether one is DPP, MCP or PP, all sane people can see that this government has failed. Even some notable DPP die hard are acknowledging that their party has failed to find solutions to the country and what they are waiting for is 2019 to come for next elections so that another can take over.
Tili nanu limodzi abale a ku Rumphi,kunonso munva posachedwapa tichita ziwonetselo.
Chifukwa tikamayankhula APM AKUMAPHWISA mwano ali ngwe ngwe ngwe ndipo fwe fwe fwe.
Tiyeni nawo amenewa zitsiru za anthu plus peter yomweyo alilephera dzikoli
Malawians will cry until their eyes will become red. Our President is still busy with his Eastern friends from China. So Malawians please keep crying.
Allan Chiyembekeza mbuzi
Jappie Mhango mbuzi
Peter Kupalamule mbuzi
George chaponda mbuzi
Henry Mussa mbuzi
Jean Kalirani mbuzi
Patricia Kaliati mbuzi
Goodall Gondwe
Ndi mbuzi zina zonse, zimene sindinazitchule koma zili boma , this is not good at all.
Ichi ndichiyambi chabe a Malawi simunati. Ife tinanena mavotavota anuwa ndizimenezotu. Malawians will die and innocent people for that matter. Lets wait and see.