Bungwe lobwerekesa ndalama la NEEF lapempha Akhristu mdziko muno kuti azibwedza ngongole

Bungwe la boma lobweleketsa ngongole la (NEEF) lapempha a khristu kuti adzibweza ngongole zomwe amatenga ku bungweli komanso mabungwe ena opereka ngongole.

Mmodzi mwa akuluakulu owona nkhanizi a Humphrey Thondolo, ndiye wanena izi Lamulungu madzulo pa mpingo wa Area 25 Assemblies of God pa maphunziro okhudza mene ndondomeko ya ngongole imayendera.

 

Malinga ndi a Thondolo maphunzirowa athandiza mamembala a mpingowu kumvetsetsa zokhudza ndondomeko ya ngongole.

 

M’busa wa mpingo wa Area 25 Asemblies of God Dr. Jim Bottoman Mbewe kubweza ngongole kaamba koti ndi mbali imodzi ya chiphunzitso cha chikhrisitu.

 

Membala wa mpingowu a Maud Gausi wati maphunzirowa abwera mu nthawi yake kutengeraso mavuto azachuma omwe akuta dziko lino.

 

Follow and Subscribe Nyasa TV :

Sharing is caring!

Follow us in Twitter
Read previous post:
Govt delay to table Judicial Service Administration bill worries Malawi Law Society

The Malawi Law Society (MLS) says the delay in tabling the Constitution (Amendment) Bill alongside the Judicial Service Administration Bill...

Close