Chipani cha DPP chikuti a Chakwera ndi munthu wabodza lankunkhuniza

Chipani chotsutsa boma cha DPP chati mtsogoleri wadziko lino Lazarus Chakwera ndimunthu wabodza lankunkhuniza.

Navicha: 

Izi zadza pamene Chakwera lero anali mnyumba yamalamulo kuyankha mafunso a aphungu.

Poyankhula ndi MIJ Online, Mary Navicha mtsogoleri wa DPP mnyumba yamalamulo wati Chakwera zonse zimene wayankhula ndizabodza kamba koti anthu akugona ndinjala komanso ali paumphawi wazaoneni.

Navicha wati ngati Chakwera akufuna apite Madera monga akumudzi akaone mmene anthu akugonela madeya.

Follow and Subscribe Nyasa TV :

Sharing is caring!

Follow us in Twitter
Read previous post:
President Chakwera says Malawi Gold hits at accumulated total value of K22Bn

Malawi President Dr Lazarus McCarthy Chakwera has disclosed that Malawi has currently accumulated Gold worth K22Billion since Government designated the...

Close