Khuda’s wife dropped from Malawi squad

Wife to South Africa-based Malawian controversial forward Khuda Muyaba, Enelecio Mhango, a national women’s football team striker, has been dropped from the Malawi squad that will go into  training camp from Friday  in preparation for Cosafa Championship.

Khuda’s wife not in the squad

She recently sparked a row on the local football scene following her rants against the Malawi national football technical panel for leaving out her husband from the squad, accusing it of forcing players to pay bribes to be considered for call-ups.

Mhango, who was part of the Scorchers’ squad in the Olympics campaign, took her frustrations to her WhatsApp status: “Nkhanza mukupangazi musaiwale nanu muli ndi ana. Zidzawaonekera hehehe agalu inu mxiew! Tomorrow don’t claim that he is from Malawi, tizakulodzani apusi inu. Nsanje ngati amadya kwanu. Kapena ndi m’bale wanu? Zautsilu.

Nde mwatengazo ndi zakhalidwe? Paja mumakonda chinyengo, mumafuna kuhongedwa. Iyaa sangayipereketu ndalama yake. Thukuta lake adye wina? Kupusa basi. Ndipo kwatsala tikutchulani maina muonekera ng’amba akadzidzi inu.”

In another status, Mhango went personal, showering insults at Flames coach Meck Mwase.

“Meck Mwase ndiwe galu, chitsiru ndi panel yako yonse simutha mpira and sizampirayi. Ndiye mwatengazo ndizabwino zoti zingapose iyeyo? Mukupanga zachimidzi apusi inu. Mukupangira chidani or what? Mudzafa ngati udzudzu mukupanda kusamala,” the status reads.

But National Women’s Football Association chairperson Suzgho Ngwira said the player has a given birth hence will not be available at Mpira Village for the training camp.

Ngwira said the striker never participated towards the end of the league and national championship play offs.

Follow and Subscribe Nyasa TV :

Sharing is caring!

Follow us in Twitter
12 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
Gee
Gee
3 years ago

Kodi a Malawi azanga ndifunseko, team yathu ya the Flames imatipindulira chani? Osangoyithetsa bwanji, akupindula ndi Walter ndi mbava zinzake mmalo mwa ma players

Ntha.....
Ntha.....
3 years ago

Shaaa

KotiMan
KotiMan
3 years ago

Inde walalata but, zomwe wanenazo zowona. Corruption yafikapo

Robert
Robert
3 years ago
Reply to  KotiMan

Ndipo kwambiri

Alamu pumani
Alamu pumani
3 years ago

A family of imbeciles. They think they are more deserving into the national team than anyone else.

Vitu Mnyenyembe
Vitu Mnyenyembe
3 years ago

Karim Benzema has been being dropped many many times in French national football team in which presumably called personal reasons with Deschamps but we have never heard such nosense like that

Last edited 3 years ago by Vitu Mnyenyembe
gangaz
gangaz
3 years ago

Team iyi angoisiya akungodya misonkho ya2 palibe chomwe apanga awawa….akulandila ma allowance a zii…team ya zbambo ndi azmay….

Ida
Ida
3 years ago

Mu banja ili mukufunika mapemphero

Chisale
Chisale
3 years ago

Typical woman, ranting at a man and the feminist think she is cool. Total disgrace.

Mulopwana
3 years ago

Mayi uyu ndi wamwano. Asazamutengenso ndi mamuna wakeyo. They have grudges amd a hammer to strike that they wil nevee pull the same direction with everyone

Dr.
Dr.
3 years ago
Reply to  Mulopwana

Ndipo sukunamadi.

Kombozo
Kombozo
3 years ago
Reply to  Mulopwana

banja limeli lisiyeni lizipanga zawo. azapha munthu anthuwa ndithu

Read previous post:
Does Mutharika really deserve peace- award, or should be General Nundwe

News in town is that former president Peter Mutharika has been named as this year’s recipient of the Uhuru/Raila Peace-Accord...

Close