Kunkuyu to deputise Msonda as PP spokesman

Malawi’s opposition Peoples party (PP) has appointed former minister of Information in the Dr Joyce Banda led government, Moses Kunkuyu as its deputy national publicity secretary.

Kunkuyu:  Deputy spokesman of PP
Kunkuyu: Deputy spokesman of PP

PP spokesman Ken Nsonda confirmed to Nyasa Times that Kunkuyu will be his deputy.

According to Nsonda, the party’s politburo meeting held in December 2014 approved the appointment of Kunkuyu to that position.

Follow and Subscribe Nyasa TV :
Follow us in Twitter

30 replies on “Kunkuyu to deputise Msonda as PP spokesman”

  1. PP a party without leadership, waiting for Roy Kachale to succeed his mother as the party president in the next general elections, a family party with no following.

  2. Moses Kunkuyu,Moses Kunkuyu,Moses Kunkuyu,how many times did I call you? Usataye nthawi ayise ndi chipani chimenechi, chinatha ngati makatani,ngakhale ayini ake amaziwa, nkowona mfundo yawo akuwuza kuti tikapanga ma Demo. Koma iwe tsiku la lero nkumati PP, suli siliyasi ayise, tawafuse anzako monga achina Kutsaira,Zulu akuwuza,asiyire a bwenubwenu ndi chipani chawo,iwe inaona kuti chipani cha anthu amenewa chikupita patali, ufuna uzimenya nkhondo yoti sukuiziwa .Uisova ayise,kapena ungodya nawo za cashgate uzawathawe cha ma 2018

  3. A Mozyy dera muliro pp mungochedwa nayo pezani zochita zina vuto sinu koma jb sadakuthangateni nthawi yomwe munali mp kumeneko ndi MCP basi kaya musova kwinako ndangodutsamo

  4. Tsobola wakale uyu suwawa,Joyce Banda 2019,kuti?kumandatu kumeneko,ku Malawi konkuno?forget!about that..kawiriso,lock aseguke,chuma chibedweso chadziko,azimai nthawi yawo atakateso,zautsiru izo

  5. MCP and PP are the parties going forward. DPP is a party of robbers, and panga thugs, UDF is a family party and it will be binned in 2019

    1. Iwe (ujeni)
      zipani zimayendesedwa ndi mbava iwe sukuziwa, ngati zikukuwawa izi tsekula mmimba mene ungathere, dpp woyeee.
      PP
      burried 18 milliom miles down the soil, lol. Ndipo sizabwereranso

  6. Mbuzi ya munthu,iwenso ndiye Crook otheratu Kunkuyu.Zoona iwe kunama kuti anthu akuba ili njira yoti upezerepo campaign kkkkkk mapwara ako ndithu ndi Nsonda yomweyo.

  7. Koma ndiye kukwera yakuphwatu, masiku alero lino pakana munthu wanzeru nzake nkumati cashgate party, chipani chopanda msogoleri,ati msogoleri nkukhala siketi, koma abale,zomvesa chisoni, ndevu pepeya pepeya pambuyo pa siketi, zausiru. Iwe Kunkuyu asiyire achina Mtambo , Msonda, Shaba, Mkandawire, Mithi, Nyirenda, chipani chawo, mwana wopenga wapanga bwanji

  8. All this time osatiuza bwanji? Kodi a Kunkuyu Ambulance yanu ya campaign iri kuti pano pa patient akuifuna ku Dedza mukapange “supplement” on government’s resources!

Comments are closed.